Mwezi wa Zul Hijjah uli mgulu la miyezi inayi yopatulika ya kalendala ya Chisilamu. Miyezi inayi yopatulika imeneyi ndi Zul Qa’dah, Zul Hijjah, Muharram ndi Rajab. Malipiro a ntchito zabwino zochitidwa m’miyezi imeneyi amachulukitsidwa, ndipo machimo amene achitidwa m’miyezi imeneyi nawonso amatengedwa kuti ndi oipitsitsa kwambiri. Allah Ta’ala akuti: إِنَّ …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu