Zizikiro za Qiyaamah

Zizindikiro za Qiyaamah

Mma hadith odalitsika, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adalosera zizindikiro zomwe zidzachitike Qiyaamah isanafike. Adauchenjeza Ummah za mayesero ndi masautso osiyanasiyana omwe adzawapeze m’malo osiyanasiyana komanso pa nthawi zosiyanasiyana pa dziko lapansi. Adawasonyezanso njira ya chiongoko ndi chipulumutso ku fitnah. Uku ndiye kukongora kosayerekezeka ndi kupambana kwa Dini ya Chisilamu …

Read More »