Zizindkiro za Qiyaamah

Momwe Adabadwira Nabi Isa (‘alaihis salaam)

Dongosolo la Allah Ta‘ala, kukamba momwe amalengedwera anthu, ndilakuti anthu awiri akakumana munthu amapangidwa. Chinthu choyamba ndi kudzera mwa makolo omwe mbewu ya mwamuna imabzalidwa m’mimba mwa mayi. Chinthu chachiwiri ndi mzimu omwe umalowa m’mimba mwa mwana yemwe sanabadweyo akakwanitsa miyezi inayi. Munthu aliyense amene anabwera padziko lapansi adatsatira njira …

Read More »

Nabi Isah ‘alaihis salaaam

Isa (‘alaihis salaam) ndi Mtumiki wa Allah Ta‘ala ndipo ali m’gulu la Aneneri apamwamba. Allah Ta‘ala adamuvumbulutsira Injeel (Baibulo) ndipo adamudaritsa ndi Shari’ah. Iye ndi Nabi amene anatumizidwa padziko lapansi Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) asanabwere. Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adati, “Ambiyaa onse (‘alaihimus salaam) ali ngati ana a bambo m’modzi. …

Read More »

kupezeka Kwa Chilungamo ndi Madalitso Mkatikati mwa Ulamuliro wa Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu)

Ulamuliro wa Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu) udzakhala wa chilungamo ndi barakah (madalitso). Popeza Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu) adzasankhidwa ndi Allah Ta‘ala kuti autsogolere ummah isadafike Qiyaamah, adzatsogozedwa ndi Allah ndikuthandizidwa ndi Iye. Popeza, chisankho chilichonse chomwe adzachite chidzadzazidwa ndi zabwino ndi chilungamo. Nthawi ya ulamuliro wake, Allah Ta‘ala adzadalitsa Asilamu ndi ma …

Read More »

Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu)

Kubwera kwa Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu) ndi chizindikiro choyamba mwa zizindikiro zikuluzikulu zomwe zidzawonekere Qiyaamah isadafike. M’mahadith odalitsika ambiri, Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adalosera za kubwera kwa Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu) ku ummah uno. Allaamah Suyuuti (rahimahullah) wafotokoza kuti mahadith okhudzana ndi kubwera kwa Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu) ndi ochuluka kwambiri kotero kuti …

Read More »

Momwe Mungadzipulumutsire ku Fitnah (Mayesero)za Dajjaal

M’mahadith odalitsika, Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adaupatsa ummah mankhwala odzitetezera ku ma Fitna a nthawi zonse komanso Mayesero a Dajjaal. Zanenedwa kuti Olemekezeka Uqbah bin Aamir (radhwiyallahu ‘anhu) nthawi ina adamufunsa Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam), “Oh Rasul wa Allah (swallallahu ‘alaihi wasallam)! Kodi njira yopezera chipulumutso ndi iti (kuchokera ku …

Read More »

Kuonongeka kwa Ummah asadafike Dajjaal

Zatchuridwa mMahadith kuti Qiyaamah isanafike, khumbo lalikulu la anthu lidzakhala kudzikundikira ndi kusonkhanitsa chuma. Anthu adzachitenga chuma ngati mfungulo ya zinthu zonse zapamwamba ndi chitonthozo, khomo la zosangalatsa zamtundu uliwonse ndi zansangulutso, ndi chida chokwaniritsira zokondweretsa za thupi ndi zilakolako za dziko. Kotero, adzapereka chilichonse kuti apeze ndipo adzachita chilichonse …

Read More »

Zida Zikuluzikulu za Dajjaal – Chuma, Akazi ndi Zansangulutso

Dajjaal akadzaonekera padziko, zida zikuluzikulu zomwe adzagwiritse ntchito kusocheretsera munthu ndi chuma, akazi ndi zansangulutso. Allah Ta’ala adzamupatsa mphamvu yochita zozizwitsa kotero kuti onse amene azidzaziona adzakopeka ndi kutengeka ndi fitnah (Mayesero) ake. Allah Ta’ala adzamloleza kugwetsa mvula, kupangitsa nthaka kutulutsa mbewu, ndipo chuma cha m’nthaka chidzamtsatira kulikonse kumene azidzapita. …

Read More »

Maonekedwe a chithupithupi cha Dajjaal

M’mahadithi olemekezeka, Olekezeka Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adatsimikizira ummah za Maonekedwe a Dajjaal a umunthu. Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kufotokoza za Dajjaal m’maonekedwe a munthu zikuonetsa kuti Dajjaal ndi munthu. Pa chifukwa chimenechi, chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah ndi chakuti Dajjaal ndi munthu, ndipo adzabwera pa dziko lapansi nthawi …

Read More »

Zizindkiro za Qiyaamah 5

Chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah pa nkhani ya Dajjaal Kutulukira komanso kubwera kwa ma fitnah a Dajjaal zimayendera limodzi m’zitaab za Aqaa’id (Zikhulupiriro za Chisilamu). Ma Ulama a Aqaa’id amavomereza kuti kukhulupirira kutulukira kwa Dajjaal ndi gawo la Aqaa’id ya Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah. Mahadith omwe mkati mwake Mtumiki …

Read More »

Zizindikiro za Qiyaamah 4

Zizindikiro Khumi Zikuluzikulu Za Qiyaamah Monga zilili kuti pali zisonyezo zambiri zing’onozing’ono za Qiyaamah zomwe zalembedwa Mmahaadith, momwemonso pali zisonyezo zikuluzikulu zambiri zomwe zatchulidwanso Mmahaadith. Zizindikiro zikuluzikulu ndi zinthu zofunikira kwambiri zomwe zidzachitike pa dziko lapansi pano Qiyaamah isanafike ndipo zidzalengeza kuyandikira kwa Qiyaamah. Ma Muhadditheen aika kubwera kwa Imam …

Read More »