M’mahadith odalitsika, Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adaupatsa ummah mankhwala odzitetezera ku ma Fitna a nthawi zonse komanso Mayesero a Dajjaal. Zanenedwa kuti Olemekezeka Uqbah bin Aamir (radhwiyallahu ‘anhu) nthawi ina adamufunsa Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam), “Oh Rasul wa Allah (swallallahu ‘alaihi wasallam)! Kodi njira yopezera chipulumutso ndi iti (kuchokera ku …
Read More »Kuonongeka kwa Ummah asadafike Dajjaal
Zatchuridwa mMahadith kuti Qiyaamah isanafike, khumbo lalikulu la anthu lidzakhala kudzikundikira ndi kusonkhanitsa chuma. Anthu adzachitenga chuma ngati mfungulo ya zinthu zonse zapamwamba ndi chitonthozo, khomo la zosangalatsa zamtundu uliwonse ndi zansangulutso, ndi chida chokwaniritsira zokondweretsa za thupi ndi zilakolako za dziko. Kotero, adzapereka chilichonse kuti apeze ndipo adzachita chilichonse …
Read More »Zida Zikuluzikulu za Dajjaal – Chuma, Akazi ndi Zansangulutso
Dajjaal akadzaonekera padziko, zida zikuluzikulu zomwe adzagwiritse ntchito kusocheretsera munthu ndi chuma, akazi ndi zansangulutso. Allah Ta’ala adzamupatsa mphamvu yochita zozizwitsa kotero kuti onse amene azidzaziona adzakopeka ndi kutengeka ndi fitnah (Mayesero) ake. Allah Ta’ala adzamloleza kugwetsa mvula, kupangitsa nthaka kutulutsa mbewu, ndipo chuma cha m’nthaka chidzamtsatira kulikonse kumene azidzapita. …
Read More »Maonekedwe a chithupithupi cha Dajjaal
M’mahadithi olemekezeka, Olekezeka Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adatsimikizira ummah za Maonekedwe a Dajjaal a umunthu. Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kufotokoza za Dajjaal m’maonekedwe a munthu zikuonetsa kuti Dajjaal ndi munthu. Pa chifukwa chimenechi, chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah ndi chakuti Dajjaal ndi munthu, ndipo adzabwera pa dziko lapansi nthawi …
Read More »Zizindkiro za Qiyaamah 5
Chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah pa nkhani ya Dajjaal Kutulukira komanso kubwera kwa ma fitnah a Dajjaal zimayendera limodzi m’zitaab za Aqaa’id (Zikhulupiriro za Chisilamu). Ma Ulama a Aqaa’id amavomereza kuti kukhulupirira kutulukira kwa Dajjaal ndi gawo la Aqaa’id ya Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah. Mahadith omwe mkati mwake Mtumiki …
Read More »Zizindikiro za Qiyaamah 4
Zizindikiro Khumi Zikuluzikulu Za Qiyaamah Monga zilili kuti pali zisonyezo zambiri zing’onozing’ono za Qiyaamah zomwe zalembedwa Mmahaadith, momwemonso pali zisonyezo zikuluzikulu zambiri zomwe zatchulidwanso Mmahaadith. Zizindikiro zikuluzikulu ndi zinthu zofunikira kwambiri zomwe zidzachitike pa dziko lapansi pano Qiyaamah isanafike ndipo zidzalengeza kuyandikira kwa Qiyaamah. Ma Muhadditheen aika kubwera kwa Imam …
Read More »Zizindikiro za Qiyaamah 3
Zizindikiro Zing’onozing’ono kuchuluka Pambuyo pa Zizindikiro Zikuluzikulu Ukawona zisonyezo zing’onozing’ono za Qiyaamah zomwe zidalembedwa Mmahaadith, munthu atha kuzindikira kuti ndi chiyambi cha kubwera kwa zisonyezo zikuluzikulu. Choncho, zoona zake ndi zoti, zizindikiro zing’onozing’ono zizidzaonjezereka pang’onopang’ono, mpaka pamapeto pake, zidzafika pachimake pa kubwera kwa zizindikiro zikuluzikulu. M’mahadith ena, Mtumiki (Swalla Allaahu …
Read More »Zizindikiro za Qiyaamah 2
Cholinga Choufotokozera Ummah Zizindikiro za Qiyaamah Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adaufotokozera Ummah za zisonyezo zing’onozing’ono ndi zikuluzikulu zomwe zidzaonekere Qiyaamah isanabwere. Zambiri mwa zizindikiro zing’onozing’ono zakhala zikuonekera kale m’zaka mazana ambiri zapitazo, pamene zambiri mwa zizindikirozi zikuchitiridwa umboni lerolino. Aalim wina yemwenso ndi Muhaddith, Allaamah Qurtubi (rahimahullah), watchula zifukwa …
Read More »Zizindikiro za Qiyaamah 1
Mma hadith odalitsika, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adalosera zizindikiro zomwe zidzachitike Qiyaamah isanafike. Adauchenjeza Ummah za mayesero ndi masautso osiyanasiyana omwe adzawapeze m’malo osiyanasiyana komanso pa nthawi zosiyanasiyana pa dziko lapansi. Adawasonyezanso njira ya chiongoko ndi chipulumutso ku fitnah. Uku ndiye kukongora kosayerekezeka ndi kupambana kwa Dini ya Chisilamu …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu