Ubwino Wopanga Salaam Choyamba Olemekezeka Abdullah bun Masuud (Allah asangalale naye) akusimba kuti Rasulullah (madalitso ndi mtendere zikhale pa iye) adati: “Amene amayambilira kupereka Salaam ndi osadzitukumura.”[1] Njira yokhanzikitsira Chikondi Olemekezeka AbuHurairah (Allah asangalale naye) akusimba kuti Rasulullah (madalitso ndi mtendere zipite kwa iye) adati: “Simudzalowa ku Paradiso pokhapokha mutakhala …
Read More »Salaam
Salaam ndi moni wa Chisilamu. Monga momwe Chisilamu chimatanthauza mtendere, moni wa Chisilamu ndi moni wamtendere komanso ofalitsa uthenga wamtendere. Salaam ndi imodzi mwa zochitika zachisilamu zomwe ndi chizindikiro cha Msilamu, ndipo kufunika kwake kwatsindikitsidwa kwambiri mahadith. Olemekezeka Abdullah bin Salaam (Radhwiyallahuanhu) akuti: Mtumiki (madalitso ndi mtendere zikhale pa iye) …
Read More »Kutonthoza Oferedwa
13. Sizoloredwa kupita ku nyumba ya kafiri yemwe wamwalira kukapepesa mwambo wamaliro uli mkati. Koma akakhala kuti ndi kafiri oyandikana naye nyumba kapena kaafir aliyense amene wataya wachibale wake, mwachitsanzo, mwana, ukhoza kumutonthoza ndi mawu awa: أَخْلَفَ اللّه عَلَيْكَ خَيْرًا مِنْهُوَاَصْلَحَكَ Akhlafa Allahu ‘Alayka Khayran Minhu Wa ‘Aslahaka Allah akupatse …
Read More »Kutonthoza Oferedwa
7. Nkoloredwa kuyamikira omwalirayo. Komabe, pomutamanda, onetsetsani kuti simukukokomeza kapena kumutamanda pa makharidwe amene panalibe mwa iye. Momwemonso musatengere chikharidwe ndi njira za makafiri pomutamanda. 8. kuchuluka kwa nthawi ya ta’ziyat ndi masiku atatu kuchokera tsiku lomwalira. Pambuyo pa tsiku lachitatu, ndi makruh kupanga ta’ziyat. Komabe, ngati munthu sadathe kubwera …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Yochezera Ndi Namfedwa
1. Ta’ziat imatanthauza kugawana chisoni ndi ananfedwa ndi kuwamvera chisoni pa kutaika kwa okondedwa wawo. Izi zimachitika pomupangira dua omwalirayo pamaso pa akubanja ake. Momwemonso izi zidzachitika polipangira Dua banja lake, kupempha Allah Odalitsika ndi Wapamwambamwamba, kuti awadalitse powapatsa kupilira ku mayesero amenewa. 2. Dua ingachitike m’mawu awa: “Allah amupatse …
Read More »Kutonthoza Oferedwa
Chisilamu ndi njira yokwanira komanso yangwiro ya moyo yomwe yaganizira zosowa zonse za munthu. Sizinangosonyeza njira ya mtendere m’moyo wa munthu, komanso zasonyeza mmene tingasonyezere chikondi ndi mtendere munthu akamwalira. Choncho Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adausonyezera Ummah momwe ungatonthozere ndi kuwapepesa ofedwa amene ali m’masautso. Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati: …
Read More »Maduwa Oyenera Kupanga Ukakamuona Odwala
Dua Yoyamba لا يَأْسَ طَهُورٌ إِنْ شَاءَ الله Palibe chifukwa chodera nkhawa, insha-Allah kudzera m’matendawa, muyeretsedwa. (i.e. Palibenso chifukwa chilichonse choti mude nkhawa kapena kuchita mantha. Mukungoyeretsedwa ku Uzimu, mukuyeretsedwa ku machimo anu, ndipo kuthupi, thupi lanu likuyeretsedwa ku poizoni. Choncho, pamene matenda abwera kwa inu ngati chifundo chobisika kumbali …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Yokaonera Odwala 2
4. Mukamayendera odwala, pemphani dua iyi: لا بَأْسَ طَهُورٌ إِنْ شَاءَ اللهُ Palibe chifukwa chodera nkhawa, insha-Allah kudzera mu matendawa, muyeretsedwa. Mukhozanso kubwereza dua iyi kasanu ndi kawiri: أَسْأَلُ اللهَ الْعَظِيمَ رَبَّ الْعَرْشِ الْعَظِيمِ أَنْ يُشْفِيكَ Ndikumupempha Allah Wamphamvu zoposa, Mbuye wa Mpando Wachifumu waukulu, kuti akuchizeni. عن ابن عباس …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Yokaonera Odwala
1. Ndi mustahab (zofunika kwambiri) kupanga wudhu usanakamuyendere odwala.[1] Olemekezeka Anas Radhwiyallahu anhu akusimba kuti Rasulullah swallallahu alaihi wasallam adati; “Amene wapanga wudhu wangwiro (pokwaniritsa masunnah ndi ma mustahab onse a wudhu) ndi kupita kukacheza ndi m’bale wake wachisilamu yemwe akudwala ndi chiyembekezo cholandira malipiro oyendera odwala, munthu oteroyo adzaikidwa …
Read More »Ubwino Oyendera Odwala 2
Kutalikitsidwa ndi Jahannam kwa ntunda okwana kuyenda zaka makumi asanu ndi awiri (70) Olemekezeka Anas (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Amene wapanga wudhu olongosoka (pokwaniritsa masunnah ndi ma mustahabbaat) ndi kupita kukamuona m’silamu nzake yemwe akudwala ndi chiyembekezo choti adzalandire malipiro okayendera nsilamu odwala, munthu oteroyo …
Read More »