Masunna Ndi Aadaab (Miyambo)

Masunnah Ndi Miyambo Ya Pakudya 2

Ma Sunnah Ena Onse ndi Aadaab Okhudzana ndi Kudya 1. Musachidandaule kapena kuchipezera vuto chakudya. Olemekezeka Abu Hurairah radhwiyallahu anhu akunena kuti Rasulullah swallallah alaihi wasallam sanachipezereko vuto chakudya. Ngati akufuna kudya ankadya, ndipo ngati sanachifune ankachisiya (popanda kuchipezera vuto). 2. Musadye chakudya chotentha kwambiri. Olemekezeka Asmaa bint Abi Bakr …

Read More »

Masunnah Ndi Miyambo Ya Pakudya 2

Ma Sunnah ndi Miyambo Musanadye 5. Sambani m’manja musanayambe kudya. Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhwiyallahu anhuma) akusimba kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati: Kusamba m’manja usanayambe kudya komanso ukamaliza kumachotsa umphawi, ndipo ndi zochokera mu sunnah ya Ambiya onse (alaihimus salaam). 6. Ndibwino kuti kuvula nsapato usanayambe kudya. Olemekezeka Anas …

Read More »

Kudya

Chisilamu ndi Dini ya padziko lonse. Ndi ya nthawi zonse, malo onse ndi anthu onse. Ndi yangwiro komanso yokwanira, kotero kuti yamuonetsa munthu njira yokwaniritsira malamulo a Allah ndi ufulu wa akapolo ake. Munthu asadafike m’dziko kufikira kumwalira, Chisilamu chakhazikitsa malamulo ndi ziletso zomwe zingamuchititse kuti akhale osangalala. Kupatura kupemphera …

Read More »

Sunnats Ndi Aadaab Za Mwezi Wa Zul Hijjah

1. Mulimbikire kuchita ibaadah m’masiku khumi oyambirira a Zul Hijjah. Malipiro aakulu atchulidwa pa ibaadah yomwe ingachitike m’masiku khumi amenewa. Olemekezeka Abdullah bin Abbaas radhwiyallahu anhu wanena kuti Nabiy swallallahu alaihi wasallam adati: “Palibe cholungama chomwe chingachitike tsiku lililonse la chaka chomwe chili chabwino kwambiri kuposa masiku khumi a mwezi …

Read More »

Zul Hijjah

Mwezi wa Zul Hijjah uli mgulu la miyezi inayi yopatulika ya kalendala ya Chisilamu. Miyezi inayi yopatulika imeneyi ndi Zul Qa’dah, Zul Hijjah, Muharram ndi Rajab. Malipiro a ntchito zabwino zochitidwa m’miyezi imeneyi amachulukitsidwa, ndipo machimo amene achitidwa m’miyezi imeneyi nawonso amatengedwa kuti ndi oipitsitsa kwambiri. Allah Ta’ala akuti: إِنَّ …

Read More »

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 4

11. Werengani durood mochuluka. Olemekezeka Aws bin Aws radhwiyallahu anhu akufotokoza kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Masiku abwino kwambiri ndi tsiku la Jumuah. 12. Yesetsani kuwerenga duruud chikwi chimodzi (ka 1000) tsiku la Jumuah. Olemekezeka Anas radhwiyallahu anhu akusimba kuti Mtumiki swallallahu alaihi wasallam adati: “Amene amawerenga duruud pa …

Read More »

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 3

9. Ngati n’kotheka, yendani wapansi popita ku musjid kukaswali swalaah ya Jumu’ah. Phanzi lirilonse lomwe mungaponye, mudzalandira mphotho ya kusala kudya kwa chaka chimodzi ndi Tahajjud. Olemekezeka Aws bin Aws Thaqafi radhwiya-Allah anhu akuti, “Ndidamva Rasulullah swallallahu alaihi wasallam akunena kuti, ‘Munthu amene amachita ghusl tsiku la Jumu’ah ndipo amapita …

Read More »

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 2

8. Pitani mwamsanga ku mzikiti kukaswali Jumu’ah, momwe mungapitire mwamsanga ndi momweso mungalandilire mphotho yochuluka. Olemekezeka Abu Hurairah radhwiya-Allahu ‘anhu akusimba kuti Rasulullah swallallahu alaihi wasallam adati, “Amene amasamba ngati momwe amasambira akakhala ndi janaabah (i.e. amasamba mosamaritsa monga momwe amachitira akakhala ndi janaabah), ndikupita ku Jumu’ah Salaah moyambilira, amalandira …

Read More »

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 1

1. Werengani Surah Dukhaan Lachinayi usiku. Olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallah anhu) akunena kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati, munthu amene amawerenga Surah Haa-meem Ad-Dukhaan usiku wa Jumu’ah ( Lachinayi usiku), machimo ake adzakhululukidwa.” 2. Sambani (ghusl) Lachisanu. Munthu amene amasamba Lachisanu, machimo ake ang’onoang’ono amakhululukidwa. Olemekezeka Abu Bakr Siddeeg (radhwiyallahj …

Read More »

Ubwino wa Jumuah

Kukhululukidwa Kwa Machimo kudzera mukuswali Jumuah Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Machimo omwe achitika pakati pa Jumu’ah ziwiri, ngati sali machimo akuluakulu, Allah amakhululuka. Tsiku Lopatulika kwa Okhulupirira Ibnu Abbaas (radhwiyallahu anhuma) adanena kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Tsiku ili (tsiku la Jumu’ah) …

Read More »