Masunna Ndi Aadaab (Miyambo)

Sunnats Ndi Aadaab Pa Kumwa 2

7. Osamwera mbali yomwe ndi yodulidwa kapena yosweka ya chikho, chifukwa ndizotheka kuti mutha kuvulala. Olemekezeka Abu Sa’eed Khudri (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adamuletsa munthu wina kumwera mbali ya chikho yophwanyika kapena kusweka. 8. Musauzire m’pweya m’chiwiya. Sayyiduna Ibnu Abbaas (radhwiyallahu anhuma) akunena kuti Rasulullah (swallallahu …

Read More »

Sunnats Ndi Aadaab Pa Kumwa 1

1)Musanamwe, Nenani dzina la Allah powerenga بِسْمِ الله M’dzina la Allah. 2) Imwani ndi dzanja lamanja. Olemekezeka Ibnu Umar radhwiyallah anhuma akunena kuti Rasulullah adati, “Aliyense wa inu akamayamba kudya, ayenera kudyera dzanja lake lamanja, ndipo akamamwa, ayenera kumwera dzanja lake lamanja, pakuti Shaitaan amadya ndi dzanja lake lamanzere ndi …

Read More »

Kumwa

Pali ma sunnah ndi ma adaab ambiri okhudzana ndi kumwa. Ma sunnah ndi ma adaab ena amakhudzana ndi madua osiyanasiyana omwe alamulidwa kuti awerengedwe usanayambe kumwa, pamene ukumwa komanso utamaliza. Ma sunnah ndi ma adaab ena amakhudzana ndi momwe munthu angamwere. Kupatula izi, pali ma sunnah ndi ma adaab omwe …

Read More »

Ma Dua Onena Ukamaliza Kudya 2

Dua 6 اَلْحَمْدُ للهِ الَّذي أَطْعَمَ وَلَا يُطْعَمُ مَنَّ عَلَيْنَا فَهَدَانَا وَأَطْعَمَنَا وَسَقَانَا وَكُلُّ بَلاَءٍ حَسَنٍ الحَمْدُ لِلهِ الَّذِي أَطْعَمَ مِنَ الطَّعَامِ وَسَقَى مِنَ الشُّرْبِ وَكَسَا مِنَ الْعُرۡيِ وَهَدٰى مِنَ الضًّلاَلَةِ وَبَصَّرَ مِنَ العَمٰي وَفَصَّلَ عَلٰى كَثِيرٍ مِمَّنْ خَلَقَ تَفْضِيْلاً ألْحَمْدُ للهِ رَبِّ الْعَالَمِين Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene …

Read More »

Ma Dua Onena Ukamaliza Kudya

Dua Yoyamba اَلْحَمْدُ لِله الَّذِي أَطْعَمَنَا وَسَقَانَا وَجَعَلَنَا مُسْلِمِينَ Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene watipatsa chakudya ndi chakumwa ndi kutipanga kukhala Asilamu. Dua Yachiwiri الْحَمْدُ لِلَّهِ الَّذِي أَطْعَمَنِيْ هَذَا الطَّعَامَ وَرَزَقَنِيْهِ مِنْ غَيْرِ حَوْلٍ مِّنّّي وَلاَ قُوَّةٍ Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene wandipatsa chakudya ichi kuti ndidye, ndipo …

Read More »

Masunnah Ndi Miyambo Ya Pakudya 2

Ma Sunnah Ena Onse ndi Aadaab Okhudzana ndi Kudya 1. Musachidandaule kapena kuchipezera vuto chakudya. Olemekezeka Abu Hurairah radhwiyallahu anhu akunena kuti Rasulullah swallallah alaihi wasallam sanachipezereko vuto chakudya. Ngati akufuna kudya ankadya, ndipo ngati sanachifune ankachisiya (popanda kuchipezera vuto). 2. Musadye chakudya chotentha kwambiri. Olemekezeka Asmaa bint Abi Bakr …

Read More »

Masunnah Ndi Miyambo Ya Pakudya 2

Ma Sunnah ndi Miyambo Musanadye 5. Sambani m’manja musanayambe kudya. Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhwiyallahu anhuma) akusimba kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati: Kusamba m’manja usanayambe kudya komanso ukamaliza kumachotsa umphawi, ndipo ndi zochokera mu sunnah ya Ambiya onse (alaihimus salaam). 6. Ndibwino kuti kuvula nsapato usanayambe kudya. Olemekezeka Anas …

Read More »

Kudya

Chisilamu ndi Dini ya padziko lonse. Ndi ya nthawi zonse, malo onse ndi anthu onse. Ndi yangwiro komanso yokwanira, kotero kuti yamuonetsa munthu njira yokwaniritsira malamulo a Allah ndi ufulu wa akapolo ake. Munthu asadafike m’dziko kufikira kumwalira, Chisilamu chakhazikitsa malamulo ndi ziletso zomwe zingamuchititse kuti akhale osangalala. Kupatura kupemphera …

Read More »

Sunnats Ndi Aadaab Za Mwezi Wa Zul Hijjah

1. Mulimbikire kuchita ibaadah m’masiku khumi oyambirira a Zul Hijjah. Malipiro aakulu atchulidwa pa ibaadah yomwe ingachitike m’masiku khumi amenewa. Olemekezeka Abdullah bin Abbaas radhwiyallahu anhu wanena kuti Nabiy swallallahu alaihi wasallam adati: “Palibe cholungama chomwe chingachitike tsiku lililonse la chaka chomwe chili chabwino kwambiri kuposa masiku khumi a mwezi …

Read More »

Zul Hijjah

Mwezi wa Zul Hijjah uli mgulu la miyezi inayi yopatulika ya kalendala ya Chisilamu. Miyezi inayi yopatulika imeneyi ndi Zul Qa’dah, Zul Hijjah, Muharram ndi Rajab. Malipiro a ntchito zabwino zochitidwa m’miyezi imeneyi amachulukitsidwa, ndipo machimo amene achitidwa m’miyezi imeneyi nawonso amatengedwa kuti ndi oipitsitsa kwambiri. Allah Ta’ala akuti: إِنَّ …

Read More »