6. Pangani ma dua komanso azkaar musanagone; اللَّهُمَّ بِاسْمِكَ أَمُوْتُ وَأَحْيٰ O, Allah Talaa mdzina Lanu ndikufa komanso ndiuka 7. Gonerani kumanja ndikuika dzanja lanu lamanja pansi pa tsaya lanu lakumanja. Bibi Hafsah (radiyallahu anha) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) akafuna kugona, ankaika dzanja lake lamanja pansi pa tsaya …
Read More »Sunnati Ndi Adaab 1
1. Mukamaliza Swala ya Esha, musakhale kumacheza nkhani zopanda pake mmalo mwake yesetsani kugona mwachangu kuti mudzukire Tahajjud komanso Swala ya Fajr mnthawi yake. Komabe, ngati pali chifukwa chomveka, monga kukambirana ndikuchita za Dini mutha, kukambirana za malamulo a Dini mashwarah ofunikira, ndi zina zotero. ndiye kuti mudzaloredwa kuchita nawo …
Read More »Kugona
Tulo ndi chimodzi mwa zinthu zofunikira kwambiri kwa munthu aliyense, monga mmene kudya ndi kumwa zilili zofunikira kwambiri. Allah Talaa akutchula za ubwino waukulu wa tulo mu Qur’aan Majiid ponena kuti: Ndipo tidakupangirani tulo kukhala mpumulo. M’ndime ina Allah Talaa akuti: Iye ndi Yemwe adakupangirani usiku kukhala chovala (chokuphimbani ndi …
Read More »Sunnats Ndi Aadaab Pa Kumwa 2
7. Osamwera mbali yomwe ndi yodulidwa kapena yosweka ya chikho, chifukwa ndizotheka kuti mutha kuvulala. Olemekezeka Abu Sa’eed Khudri (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adamuletsa munthu wina kumwera mbali ya chikho yophwanyika kapena kusweka. 8. Musauzire m’pweya m’chiwiya. Sayyiduna Ibnu Abbaas (radhwiyallahu anhuma) akunena kuti Rasulullah (swallallahu …
Read More »Sunnats Ndi Aadaab Pa Kumwa 1
1)Musanamwe, Nenani dzina la Allah powerenga بِسْمِ الله M’dzina la Allah. 2) Imwani ndi dzanja lamanja. Olemekezeka Ibnu Umar radhwiyallah anhuma akunena kuti Rasulullah adati, “Aliyense wa inu akamayamba kudya, ayenera kudyera dzanja lake lamanja, ndipo akamamwa, ayenera kumwera dzanja lake lamanja, pakuti Shaitaan amadya ndi dzanja lake lamanzere ndi …
Read More »Kumwa
Pali ma sunnah ndi ma adaab ambiri okhudzana ndi kumwa. Ma sunnah ndi ma adaab ena amakhudzana ndi madua osiyanasiyana omwe alamulidwa kuti awerengedwe usanayambe kumwa, pamene ukumwa komanso utamaliza. Ma sunnah ndi ma adaab ena amakhudzana ndi momwe munthu angamwere. Kupatula izi, pali ma sunnah ndi ma adaab omwe …
Read More »Ma Dua Onena Ukamaliza Kudya 2
Dua 6 اَلْحَمْدُ للهِ الَّذي أَطْعَمَ وَلَا يُطْعَمُ مَنَّ عَلَيْنَا فَهَدَانَا وَأَطْعَمَنَا وَسَقَانَا وَكُلُّ بَلاَءٍ حَسَنٍ الحَمْدُ لِلهِ الَّذِي أَطْعَمَ مِنَ الطَّعَامِ وَسَقَى مِنَ الشُّرْبِ وَكَسَا مِنَ الْعُرۡيِ وَهَدٰى مِنَ الضًّلاَلَةِ وَبَصَّرَ مِنَ العَمٰي وَفَصَّلَ عَلٰى كَثِيرٍ مِمَّنْ خَلَقَ تَفْضِيْلاً ألْحَمْدُ للهِ رَبِّ الْعَالَمِين Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene …
Read More »Ma Dua Onena Ukamaliza Kudya
Dua Yoyamba اَلْحَمْدُ لِله الَّذِي أَطْعَمَنَا وَسَقَانَا وَجَعَلَنَا مُسْلِمِينَ Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene watipatsa chakudya ndi chakumwa ndi kutipanga kukhala Asilamu. Dua Yachiwiri الْحَمْدُ لِلَّهِ الَّذِي أَطْعَمَنِيْ هَذَا الطَّعَامَ وَرَزَقَنِيْهِ مِنْ غَيْرِ حَوْلٍ مِّنّّي وَلاَ قُوَّةٍ Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene wandipatsa chakudya ichi kuti ndidye, ndipo …
Read More »Masunnah Ndi Miyambo Ya Pakudya 2
Ma Sunnah Ena Onse ndi Aadaab Okhudzana ndi Kudya 1. Musachidandaule kapena kuchipezera vuto chakudya. Olemekezeka Abu Hurairah radhwiyallahu anhu akunena kuti Rasulullah swallallah alaihi wasallam sanachipezereko vuto chakudya. Ngati akufuna kudya ankadya, ndipo ngati sanachifune ankachisiya (popanda kuchipezera vuto). 2. Musadye chakudya chotentha kwambiri. Olemekezeka Asmaa bint Abi Bakr …
Read More »Masunnah Ndi Miyambo Ya Pakudya 2
Ma Sunnah ndi Miyambo Musanadye 5. Sambani m’manja musanayambe kudya. Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhwiyallahu anhuma) akusimba kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati: Kusamba m’manja usanayambe kudya komanso ukamaliza kumachotsa umphawi, ndipo ndi zochokera mu sunnah ya Ambiya onse (alaihimus salaam). 6. Ndibwino kuti kuvula nsapato usanayambe kudya. Olemekezeka Anas …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu