Sahaabah

Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) amupempha Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) kuti amuwerengere Quraan Majeed

Nthawi ina, Rasullullah (Swallallahu alaihi wasallam) anabwera ku fuko la Bani Zafar (fuko lachi Ansaar). Ali pa mimbar akulankhula nawo, anamuuza Abdullah bin Mas’ood (radhwiyallahu ‘anhu), kuti, “Ndiwerengere Quraan.” Modzichepetsa kwambiri, Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) anauza Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam), “Eh Mtumiki wa Allah, kodi ndikuwerengereni kumachita kuti Quraan …

Read More »

Chitsimikizo Cha Sayyiduna Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) Pa Mawu a Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam)

Ulendo wina, nthawi ya khilaafat yake, Sayyiduna Uthmaan (radhwiyallhu ‘anhu) anabwera kudzacheza ndi Olemekezeka Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu). Apa ndikuti Abdullah bin Masood (radhwiyallahu ‘anhu) akudwala matenda ake omaliza. Sayyiduna Uthman (radhwiyallahu ‘anhu) anamufunsa kuti, “Ndi vuto lanji lomwe likukusautsa?” Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) anayankha kuti, “Chomwe chikundisautsa …

Read More »

Hazrat Abdullah ibn Mas’uud (radhiyallahu anhu) Kuwerenga Qur’aan Majeed mokweza mawu pamaso pa Aquraish

Hazrat Abdullah ibn Mas’uud (radhiyallahu anhu) adali munthu oyamba kuwerenga Qur’aan Majeed mokweza mawu ku Makkah Mukarramah Aquraish asanalowe Chisilamu. Tsiku lina, maSwahaabah (radhiyallahu anhum) anasonkhana nati, “Ndikulumbira mwa Allah, Aquraish sanamvepo wina akuwerenga Qur’aan mokweza mawu pamaso pawo, ndiye ndani pakati pathu amene ali okonzeka kupita kukawerenga Qur’aan mokweza …

Read More »

Kulimba Mtima kwa Hazrat Abdullah bin Mas’uud (Radhiyallahu ‘anhu)

Pankhondo ya Hunain, Asilamu adagonjetsedwa kwakanthawi kochepa. Munthawi yovutayi, Hazrat Abdullah bin Mas’uud (Radhwiyallahu ‘anhu) adali m’gulu la ma swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) amene adapirirabe ndikukhala limodzi Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam). Hazrat Abdullah bin Mas’ood (radhwiyallahu ‘anhu) akufotokoza kuti: “Ndinali ndi Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) tsiku la …

Read More »

Olemekezeka Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) apha Abu Jahl

Nkhondo ya Badr itafika kumapeto ndipo Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) ndi maswahaabah atapambana, Rasulullah (sallallahu ‘alayhi wasallam) adauza ma swahaabah kuti, “Ndani atapite kukaona momwe Abu Jahl alili?” Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) adapita kukamfunafuna ndipo adapeza kuti ana awiri a ‘Afraa (radhwiyallahu ‘anha) adali atamuvulaza, ndipo anali mu ululu …

Read More »

Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu)

Olemekezeka Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) anali mnyamata wamng’ono, akuweta mbuzi za Uqbah bin Abi Mu’ait m’chigawo cha Makkah Mukarramah. Tsiku lina ali kuweta mbuzi, Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) adadutsa pamene ankathawa ma mushrikiin. Popeza chinali chizolowezi cha Aarabu kupereka mkaka kwa odutsa mnjira, Rasulullah …

Read More »

Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) Kuyamikira Kuwerenga Quran kwa Abdullah bin Mas’uud (Radhwiyallahu ‘anhu)

Umar (radhwiyallahu ‘anhu) adafotokoza nkhani iyi: Rasulullah (swallallahu ‘alayhi wasallam) ankakonda kulankhula ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) akamaliza kuswali Esha ndikukambirana naye zokhuza Asilamu. Usiku wina, atamilza swalah ya Esha, Rasulullah (sallallahu ‘alayhi wasallam) adayamba kuyankhula ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) (zokhudza Asilamu) ndipo inenso ndidali nawo pomwepo. Pambuyo pokambirana, …

Read More »

Abu Zar (radhiyallahu ‘anhu) Apereka Uphungu kwa Mtsogoleri wa Asilikali Kuti Atsatire Chilungamo

Imaam Bayhaqi (rahimahullah) akunena kuti: Yazid bin Abi Sufyaan (radhiyallahu ‘anhu) pamene adali bwanamkubwa wa Shaam, Asilamu adachita Jihaad ndipo adapambana, motero adapeza chuma cholanda kwa adani. Mkatikati mwa katundu ameneyo mudalinso mtsikana okongola yemwe adaperekedwa kwa msilikali wina wachisilamu ngati gawo lake. Msilikaliyu atangolandira gawo lakeli (mtsikananayu), Yazid bin …

Read More »

Kumwalira kwa Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu)

Olemekezeka Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu) atatsala pang’ono kumwalira, panalibe wina aliyense kupatula mkazi wake ndi kapolo wake. Anawalangiza kuti, “Mundisambitse ndi kundiveka sanda (ndikamwalira). Kenako tengani thupi langa ndi kuliyika pamsewu. Uzani gulu la anthu lomwe liyambilire kudutsa kuti, “Uyu ndi Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu),Otsatira wa Rasulullah (swallallahu ‘alayhi wasallam). …

Read More »

Olemekezeka Abu Zarr adzudzula wantchito wake

Tsiku lina munthu ochokera ku fuko la Banu Sulaim anabwera kwa Abu Zarr (radhwiyallahu anhu) ndipo anamuuza kuti: “Ndikufuna kukhala nanu kuti ndipindule ndi maphunziro anu a malamulo a Allah Ta’ala ndi ma sunnah a Nabi swallallahu alaihi wasallam Inenso ndidzathandiza wantchito wanu kusamalira ngamila.” Abu Zarr radhwiyallahu anhu anayankha …

Read More »