Nkhondo ya Badr itafika kumapeto ndipo Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) ndi maswahaabah atapambana, Rasulullah (sallallahu ‘alayhi wasallam) adauza ma swahaabah kuti, “Ndani atapite kukaona momwe Abu Jahl alili?” Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) adapita kukamfunafuna ndipo adapeza kuti ana awiri a ‘Afraa (radhwiyallahu ‘anha) adali atamuvulaza, ndipo anali mu ululu …
Read More »Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu)
Olemekezeka Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) anali mnyamata wamng’ono, akuweta mbuzi za Uqbah bin Abi Mu’ait m’chigawo cha Makkah Mukarramah. Tsiku lina ali kuweta mbuzi, Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) adadutsa pamene ankathawa ma mushrikiin. Popeza chinali chizolowezi cha Aarabu kupereka mkaka kwa odutsa mnjira, Rasulullah …
Read More »Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) Kuyamikira Kuwerenga Quran kwa Abdullah bin Mas’uud (Radhwiyallahu ‘anhu)
Umar (radhwiyallahu ‘anhu) adafotokoza nkhani iyi: Rasulullah (swallallahu ‘alayhi wasallam) ankakonda kulankhula ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) akamaliza kuswali Esha ndikukambirana naye zokhuza Asilamu. Usiku wina, atamilza swalah ya Esha, Rasulullah (sallallahu ‘alayhi wasallam) adayamba kuyankhula ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) (zokhudza Asilamu) ndipo inenso ndidali nawo pomwepo. Pambuyo pokambirana, …
Read More »Abu Zar (radhiyallahu ‘anhu) Apereka Uphungu kwa Mtsogoleri wa Asilikali Kuti Atsatire Chilungamo
Imaam Bayhaqi (rahimahullah) akunena kuti: Yazid bin Abi Sufyaan (radhiyallahu ‘anhu) pamene adali bwanamkubwa wa Shaam, Asilamu adachita Jihaad ndipo adapambana, motero adapeza chuma cholanda kwa adani. Mkatikati mwa katundu ameneyo mudalinso mtsikana okongola yemwe adaperekedwa kwa msilikali wina wachisilamu ngati gawo lake. Msilikaliyu atangolandira gawo lakeli (mtsikananayu), Yazid bin …
Read More »Kumwalira kwa Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu)
Olemekezeka Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu) atatsala pang’ono kumwalira, panalibe wina aliyense kupatula mkazi wake ndi kapolo wake. Anawalangiza kuti, “Mundisambitse ndi kundiveka sanda (ndikamwalira). Kenako tengani thupi langa ndi kuliyika pamsewu. Uzani gulu la anthu lomwe liyambilire kudutsa kuti, “Uyu ndi Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu),Otsatira wa Rasulullah (swallallahu ‘alayhi wasallam). …
Read More »Olemekezeka Abu Zarr adzudzula wantchito wake
Tsiku lina munthu ochokera ku fuko la Banu Sulaim anabwera kwa Abu Zarr (radhwiyallahu anhu) ndipo anamuuza kuti: “Ndikufuna kukhala nanu kuti ndipindule ndi maphunziro anu a malamulo a Allah Ta’ala ndi ma sunnah a Nabi swallallahu alaihi wasallam Inenso ndidzathandiza wantchito wanu kusamalira ngamila.” Abu Zarr radhwiyallahu anhu anayankha …
Read More »Abu Zarr (radhwiyallahu ‘anhu) Alemekeza kwambiri Uthmaan (radhwiyallahu ‘anhu)
Munthu wina ochokera ku fuko la Banu Sulaym adayankhula izi: “Nthawi ina ndinakhala pa gulu lomwe Abu Zarr anali pomwepo. Maganizo anga anali oti mwina Abu Zarr wamukwiyira Uthmaan (radhwiyallahu ‘anhu) chifukwa choti Uthmaan (radhiyallahu ‘anhu) adamupempha kuti asamuke ku Madinah Munawwarah ndikukakhala ku Rabadha. Pagulupo wina adapereka ndemanga yomutsutsa …
Read More »Olemekezeka Abu Zarr (radhwiyallahu ‘anhu) asamukira ku Shaam ndi Rabadhah
Zidatengera Abu Zarr Ghifaari (radhiyallahu ‘anhu) kuphunzira moyo wa Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) osasamala za moyo wadziko lapansi komanso kudziletsa ndi kumvera machenjezo amphamvu kwa omwe ali ndi chuma koma osagwiritsa ntchito moyenera, Abu Zarr (radhwiyallahu ‘anhu) adayamba kudana ndi dziko lapansi kotero kuti sanasunge chuma ndipo sankakonda kuona anthu …
Read More »Kusalilabadira kwa Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu) Ddziko Lapansi
Abu Zar Ghifaari (Radhwiyallahu ‘anhu) anali Sahaabi yemwe ankafanana ndi Nabiy Isa (‘alaihis salaam) m’maonekedwe ake komanso kukongola kwake. Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) anati, “Aliyense amene akufuna kumuona Isa bin Maryam (‘alaihis salaam) Taqwa yake, chilungamo chake, ndi kudzipereka kwake (pa ibaadah), ayenera kumuyang’ana Abu Zar” (Majmauz Zawaaid #15817) Chimodzimodzinso, …
Read More »Kutsatira kwa Abu Zar (radhiyallahu ‘anhu) Malangizo a Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam
Ma’roor bin Suwaid (rahimahullah) akufotokoza izi: Nthawi ina tinadutsa kwa Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu) ku Rabzah ndipo tinaona kuti anali atavala zovala ziwiri. Chimodzi chinali chakale, pomwe china chinali chatsopano, ndipo kapolo wake nayenso anali atavala zovala ziwiri, zomwe chimodzi chinali chatsopano ndipo china chinali chakale. Kenako tidati kwa Abu …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu