Sahaabah

Abdullah bin Abbaas Akishinda pamoja na Mtume (Sallallahu alaihi wasallam) usiku ili ajifunze swalah ya Tahajjud ya Mtume (Sallallahu alaihi wasallam)

Mjomba wake Rasulullah (Sallallahu alaihi wasallam), ‘Abbaas (Radhiya Allaahu ‘anhu), alitamani mtoto wake Abdullah bin ‘Abbaas (Radhiyallahu ‘anhuma) ashinde na Rasulullah (Sallallahu alaihi wasallam) usiku ili afaidike na ushirika wake uliobarikiwa. Katika riwaya ya Muslim na Tahaawi, Abdullah bin Abbaas (Radhiya Allaahu ‘anhuma) anataja kwamba baba yake, Abbaas (Radhiya Allaahu …

Read More »

Uphungu wa Abdullah bin Abbaas (radhiyallahu ‘anhuma)

Wahab bin Munabbih (rahimahullah) akunena kuti: Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhiyallahu ‘anhuma) atasanduka wakhungu (ku ukalamba wake), ndidamutsogolera ku Haram Sharif ku Makkah Mukarramah, komwe anamva gulu la anthu likukangana pakati pawo. Anandipempha kuti ndimulondolere kwa iwo. Atafika kwa iwo, anawalonjera ndi mawu onena kuti “Assalaamu Alaikum”. Anamupempha kuti akhale …

Read More »

kuzindikira kwakukulu kwa Abdullah bin Abbaas (radhiwyallahu ‘anhuma)

Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhwiyallahu ‘anhuma) akuti: Mtumiki wa Allah (swallallahu ‘alaihi wasallam) atamwalira, ndinauza mnzanga wina wachi Ansaari kuti, “Bwera, tiye tipite tikaphunzire (Dini) kuchokera kwa Ma Sahaabah (radhwiyallahu ‘anhum), pomwe ambiri a iwo akadalipo pakati pathu.” Anandiyankha kuti, “Iwe Ibnu Abbaas! Ndikulumbira mwa Allah, ndikudabwa kuti ukuganiza kuti …

Read More »

Kachitidwe ka Mu’aaz (radhiyallahu ‘anhu) Kuwerenga Quraan Majeed pa Tahajjud

Mtumiki (swallallahu ‘alaihi wasallam) anatumiza Mu’aaz (radhwiyallahu ‘anhu) kuti akalamulire gawo lina la Yemen, ndipo Abu Musa Ash’ari (radhwiyalllahu ‘anhu) akalamulire gawo lina. Mtumiki (swallallahu ‘alaihi wasallam) anawalankhula ndipo anawapatsa uphungu otsatirawu asanawatumize. Anawauza kuti, “Fewetsani zinthu (kwa anthu), ndipo musawakhwimitsire. Perekani uthenga wabwino (kwa anthu), ndipo musawathamangitse (ku dini).” …

Read More »

Ubale Wapafupi Umene Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) Anasangalala Nawo Ndi Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam)

Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) akunena kuti, “Nthawi ina, ndinali nditakhala kumbuyo kwa Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) pa bulu pamene naye analinso pomwepo. Panalibe chilichonse pakati pa ine ndi Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kupatula thabwa la chokhalira (chomwe chimalekanitsa okwera ndi munthu amene wakhala kumbuyo kwake). “Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) …

Read More »

Malangizo Otsanzikirana a Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kwa Mu’aaz (radhwiyallahu ‘anhu) pamene ankamutumiza ku Yemen

Pamene Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) ankatumiza Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) ku Yemen kuti akaphunzitse anthu dini ndikuwalamulira, posiyana naye, Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) ankayenda naye mpaka kunja kwa mzinda wa Madinah Munawwarah pamene ankamupatsa uphungu osiyanirana. Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) anamulamula kuti achite zinthu zina zabwino, ndipo anamulamula kuti …

Read More »

Kumapeto Kwa Moyo Wa Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) Padziko Lapansi

Mtumiki (swallallahu ‘alayhi wasallam) adati, “Munthu amene amamwalira ndi mliri, amakhala wamwalira imfa ya shahid. Mu khilaafat ya Umar (radhwiyallahu ‘anhu), mliri wa Amwaas unakhudza Shaam m’chaka cha 17 pambuyo pa Hijrah. Mu mliriwu Abu Ubaidah (radhwiyallahu ‘anhu), mtsogoleri wa Asilamu ku Shaam, anakhudzidwa nawonso ndipo pambuyo pake anamwalira. Asanamwalire, …

Read More »

Makhalidwe Abwino a Muaaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu)

Farwah bin Nawfal akufotokoza kuti nthawi ina yake, Abdullah bin Masud (radhwiyallahu anhu) adalankhula za Muaaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) ndipo ankamuyamikira kwambiri chifukwa cha zabwino zomwe anali nazo. Iye adati: إن معاذا كان أمة قانتا لله حنيفا “Ndithu, Muaaz (bin Jabal) adali ummah (mtsogoleri wlotsogolera ena kunjira yoongoka), pomwe …

Read More »

Mtumiki (Swallallahu ‘alaihi wasallam) asankha Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) kukhala Bwanamkubwa wa Yemen

Rasulullah (Swallallahu ‘alaihi wasallam) pomutumiza Mu’aaz (radhwiyallahu ‘anhu) ku Yemen, adamufunsa kuti, “Ndi njira yanji yomwe udzatsatire ukamakapereka chigamulo pa nkhani za Asilamu?” Mu’aaz (Radhwiyallahu ‘anhu) adayankha kuti: “Ndidzagwiritsa ntchito Qur’aan.” Kenako Nabi (Swallallahu ‘alaihi wasallam) adamufunsa kuti: “Ngati lamulo silikupezeka mu Qur’aan udzatani?” Iye adayankha kuti, “Ndidzagwiritsa nctchito mahaadith …

Read More »