Monthly Archives: February 2026

Kukhala Ndi Mtima Okhululukira Ena

Olemekezeka Waa’il bin Hujr (Radhwiya-Allahu anhu) adali Swahaaba otchuka wa Rasulullah (swallallah alaihi wasallam) yemwe ankachokera dela la Yemen ndipo adali ochokera ku banja lachifumu. Zanenedwa kuti atanyamuka ku Yemen kubwera ku Madinah Munawwarah kudzalowa Chisilamu, asadafike Rasulullah Allah adawadziwitsa ma Swahaabah kuti watsala pang’ono kufika. Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) …

Read More »

Maonekedwe a Nabi Isah ‘alaihis salaam

Nabi Isa (‘alaihis salaam) anatumizidwa ndi Allah Ta‘ala kwa Bani Israa’eel. Limodzi mwa malamulo omwe Allah Ta‘ala adamupatsa linali kupereka uthenga wabwino kwa anthu ake okhudza kubwera kwa Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) padziko lapansi. Allah Ta‘ala akunena mu Qur’aan Majeed: وَ اِذۡ قَالَ عِیۡسَی ابۡنُ  مَرۡیَمَ یٰبَنِیۡۤ اِسۡرَآءِیۡلَ  اِنِّیۡ  رَسُوۡلُ  …

Read More »