Mu Quraan Majid, Tsiku la Qiyaamah latchulidwa ndi mayina osiyanasiyana. Mayina ena mwa awa ndi “Tsiku la Mphotho ndi Kubwezera”, “Tsiku losonkhana”, “Tsiku la Kutayika ndi Kupindula” (lodzataika kwa osakhulupirira ndi la phindu kwa okhulupirira), ndi “Tsiku la Kukumana” (kutanthauza kukumana ndi Allah Talaa. Tikayang’ana mayina awa, timapeza kuti dzina …
Read More »Kuyamika Pa Mdalitso Okhala Ndi Moyo
Dawuud bin Dinaar anali Imaam wamkulu pankhani ya Hadith komanso mphunzitsi wa ma Muhadditheen otchuka, monga Imaam shu’bah (rahimahullah) ndi Imaam Wakii (rahimahullah). Mkatikati mwa moyo wake kunadzabuka mliri ku Khuraasaan kumene ankakhala omwe udakhudza anthu ndipo ambiri adataya miyoyo yawo. Dawuud bin Dinaar (rahimahullah) anali m’gulu la omwe adagwidwa …
Read More »Imaam Ahmad bin Hambal (rahimahulla) Kupindura kuchoka kwa Bishr Haafi (rahimahulla)
Nkhani yotsatirayi ikuunikira kumvetsetsa kwakuya kwa dini ndi ma’rifat (kuzindikirika) ya Allah Talaa zomwe Allah Talaa adamudalitsa nazo Bishr Haafi (rahimahulla) zomwe zidachititsa kuti mpaka Imam Ahmad (rahimahulla) amutsanzire: M’nthawi ya Imaam Ahmad bin Hambal (rahimahulla) kunali dotolo wina yemwe ankatchedwa kuti Abdur Rahmaan At-Tabeeb. Ankathandiza Imaam Ahmad bin Hambal …
Read More »Munthu Olungama Kwambiri – Fudhail Bin Iyaaz Rahimahullah
Fudhail bun Iyaaz (Rahimahullah) aDali Muhaddith olemekezeka komanso oyera mtima wa m’nthawi yake. Allah Talaa adamdalitsa ndi ulemelero wapamwamba kwambiri mu Hadith kotero kuti ambiri mwa ma Muhadith otsogola, monga Abdullah bin Mubaarak, Sufyaan bun Uyainah ndi Imaam Shaafi’e (Rahimahullah) adafotokoza Hadith kuchokera kwa iye. Zanenedwa kuti Fudhail (Rahimahullah) asanadalitsidwe …
Read More »Osataya Chiyembekezo Mu Kusinthika Kwa Munthu Aliyense
Abdullah bin Maslamah Q’anabi (rahimahullah) anali m’gulu la ma Muhadditheen otsogola mu nthawi yake. Iye anali mtsogoleri wa ma Muhadditheen ambiri otchuka, ngati Imaam Bukhaari, Imaam Muslim ndi Imaam Abu Dawood (rahimahullah) Zikunenedwa kuti pachiyambi cha moyo wake, ankacheza ndi anthu oipa ndipo ankamwa mowa. Komabe, atakumana ndi Muhaddith …
Read More »Nkhani Yokhudza Kulowa Chisilamu Kwa Sayyiduna Wahshi Radhwiyallahu Anhu
Pankhondo ya Uhud, chimodzi mwa zowawa zowawitsa zomwe zidamuchitikira Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) kudali kuphedwa kwa amalume ake okondedwa Sayyiduna Hamzah (radhwiyallahu anhu) Amene adamupha Hamzah sanali wina koma Wahshi bun Harb Nthawi imeneyo ndikuti asadakhale nsilamu, koma Allah Talaa pambuyo pake adamdalitsa ndi Imaan ndi ulemelero okhala Sahaabi. Nkhani …
Read More »Ufulu Wa Anansi (Aneba)
Kuti dziko liziyenda bwino komanso mogwirizana, ndikofunikira kuti munthu aliyense alemekeze ufulu wa anthu ena. Ngati ufulu wa anthu siulemekezedwa ndi kukwaniritsidwa, ndiye kuti chisokonezo ndi mikangano zidzafalikira padziko lonse lapansi. Kuba ndi kulanda chuma kudzakhala paliponse ndipo kuponderezana ndi kuphwanya malamulo kudzakhala chinthu chotchuka kwambiri. Anthu adzapondereza ufulu wa …
Read More »Kukhala Ndi Mtima Okhululukira Ena
Olemekezeka Waa’il bin Hujr (Radhwiya-Allahu anhu) adali Swahaaba otchuka wa Rasulullah (swallallah alaihi wasallam) yemwe ankachokera dela la Yemen ndipo adali ochokera ku banja lachifumu. Zanenedwa kuti atanyamuka ku Yemen kubwera ku Madinah Munawwarah kudzalowa Chisilamu, asadafike Rasulullah Allah adawadziwitsa ma Swahaabah kuti watsala pang’ono kufika. Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) …
Read More »Kufunira Ena Zabwino
Kuchokera mu dongosolo lonse la makhalidwe abwino la Chisilamu, makhalidwe onse omwe Chisilamu chimalimbikitsa ndi odzadza ndi zokopa ndipo amawalitsa kukongola. Kaya ndi kulemekeza okalamba, kapena kuchitira chifundo achinyamata, kapena kukwaniritsa ufulu wa makolo ndi abale anu, zonse zimasonyeza ulemerero wapadera wa Chisilamu. Komabe, moyo wa makhalidwe onse apamwambawa uli …
Read More »Makolo Kutsogolera Mwa Chitsanzo
Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) anali olemekezeka kwambiri pa zolengedwa za Allah, Allah adamusankha kukhala Mtumiki Wake omaliza ndipo adamudalitsa ndi dini yolemekezeka kwambiri – dini ya Chisilamu yomwe ndi malamulo abwino kwambiri a moyo kuti munthu atsatire. Munthu akalingalira pa umunthu odalitsika wa Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) amapeza kuti Allah …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu