Paulendo wa Tabuuk, ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) adali pa ulendo ndi Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam). Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adachoka kwa ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) kuti apite kukazithandiza. Popeza kuti nthawi ya Swalah ya Fajr sidali yochuluka, ndipo ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) ankaopa kuti nthawi itha kutha, sadamudikire …
Read More »Zizindkiro za Qiyaamah 5
Chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah pa nkhani ya Dajjaal Kutulukira komanso kubwera kwa ma fitnah a Dajjaal zimayendera limodzi m’zitaab za Aqaa’id (Zikhulupiriro za Chisilamu). Ma Ulama a Aqaa’id amavomereza kuti kukhulupirira kutulukira kwa Dajjaal ndi gawo la Aqaa’id ya Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah. Mahadith omwe mkati mwake Mtumiki …
Read More »Ubwino Oyendera Odwala 2
Kutalikitsidwa ndi Jahannam kwa ntunda okwana kuyenda zaka makumi asanu ndi awiri (70) Olemekezeka Anas (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Amene wapanga wudhu olongosoka (pokwaniritsa masunnah ndi mustahabbaat) ndi kupita kukamuona m’silamu nzake yemwe akudwala ndi chiyembekezo choti adzalandire malipiro okayendera nsilamu odwala, munthu woteroyo adzaikidwa …
Read More »Olemekezeka Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) ndi mmodzi mwa Asilamu opambana.
Nthawi ina Rasulullah (Swalla-Allaahu ‘alayhi wasallam) adamufunsa Busrah bint Safwan (Radhwiya-Allahu ‘anha) kuti ndi ndani amene ankafuna kukwatira mphwake, Umm Kulthuom bint Uqbah. Adamufotokozera mayina a anthu ochepa omwe adamfunsira mphwakeyo, ndipo adamuwuzanso kuti mwa anthu omwe adamfunsira mphwakeyo ndi Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu). Zitatero, Mtumiki (Swalla-Allaahu ‘alayhi …
Read More »Ubwino Osiya Pambuyo Mwana Olungama
Bambo a Nabii Yunus (alayhis salaam) adali munthu Owopa Allah dzina lawo Mattaa. Iwo ndi mkazi wawo kwa nthawi yaitali ankafuna kuti Allah atawadalitsa ndi mwana wamwamuna ndi kumuchita kukhala Mneneri kwa Bani Israeil. Zaka zambiri zidadutsa uku akumapempha mpaka pamapeto pake adaganiza zopita kukasupe odalitsika wa Nabii Ayyoob komwe …
Read More »Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu pa Nkhondo ya Uhud
Pankhani ya kupirira kwa Talha (Radhwiyallahu ‘anhu) pankhondo ya Uhud, Sa’d bin Abi Waqqaas (Radhwiyallahu ‘anhu) adanena izi: Allah Ta’ala amuchitire chifundo Talha. Mosakayikira, mwa ife tonse, adamuthandiza kwambiri Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wa wasallam) pa tsiku la Uhud. Kenako Sa’d (Radhwiyallahu ‘anhu) adafunsidwa: “Tifotokozere momwe (adamuthandizira kwambiri Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi …
Read More »Ubwino Oyendera Odwala 1
Kupeza Mwayi Opangiridwa Dua Ndi Angelo Okwana Zikwi Makumi Asanu Ndi Awiri (70,000) Olemekezeka Ali (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Amene amayendera odwala m’bandakucha, angero zikwi makumi asanu ndi awiri (70,000) amamupemphera chifundo kwa Allah mpaka madzulo; Amene angamuyendere odwala madzulo angelo okwana 70,000 amamupemphera chifundo …
Read More »Mlamu wa Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam)
Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) adakwatira akazi okwana anayi. Aliyense mwa akazi ake anayi anali pachibale ndi m’modzi mwa akazi olemekezeka a Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi waaalihi wasallam). Ndichifukwa chake Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adamuuza kuti: “(Ndiwe) mlamu wanga padziko lapansi ndi tsiku lotsiriza (kutanthauza kuti udzakhalanso mlamu wanga …
Read More »Kuyendera Odwala
Chipembedzo cha Chisilamu chimalimbikitsa ndi kulamula kuti munthu akwaniritse udindo umene ali nawo kwa Allah ndi udindo umene ali nawo kwa akapolo a Allah. Pankhani ya udindo ndi maufulu omwe munthu ali nawo pa akapolo a Allah, izi zikhoza kugawidwa m’mitundu iwiri ya maufulu. Mtundu oyamba ndi ufulu umene uli …
Read More »Kuwolowa kwambiri manja kwa Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu)
Mkazi wa Talhah (Radhwiyallahu ‘anha), Su’da bint ‘Awf al-Muriyyah anakambapo izi zokhudza mwamuna wake Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu): “Tsiku lina Talha analowa m’nyumba ali okhumudwa. Chavuta ndi chiyani? Kodi ndalakwitsa penapake mchifukwa ndikuwona kuti mukuonetsa kukhumudwa? Chonde ndiuzeni kuti ndithe kuchotsa kukhumudwa kwanu. Iye adayankha, “Ayi, siunandilakwire chilichonse, ndipo ndithudi, ndiwe …
Read More »