Ma Ubwino Okhudza Kupereka Salaam

Ubwino Wopanga Salaam Choyamba Olemekezeka Abdullah bun Masuud (Allah asangalale naye) akusimba kuti Rasulullah (madalitso ndi mtendere zikhale pa iye) adati: “Amene amayambilira kupereka Salaam ndi osadzitukumura.”[1] Njira yokhanzikitsira Chikondi Olemekezeka AbuHurairah (Allah asangalale naye) akusimba kuti Rasulullah (madalitso ndi mtendere zipite kwa iye) adati: “Simudzalowa ku Paradiso pokhapokha mutakhala …

Read More »

Udindo Wapamwamba wa Olemekezeka Said bin Zaid (Radhwiya Allaahu ‘anhu) Pakati pa anthu a ku Madinah Munawwarah

M’nthawi ya khilaafah ya Olemekezeka Mu’aawiyah (Radhwiya Allahu ‘anhu) adalembera kalata Marwaan bin Hakam bwanamkubwa wake yemwe adasankhidwa ku Madinah Munawwarah pomwe adamulangiza kutenga bay’at (chikole cha chikhulupiriro) kwa anthu a ku Madinah Munawwarah m’malo mwa mwana wake, Yaziid bin Mu’aawiyah, yemwe adzakhale Khalifah m’malo mwake mwake. Mu’aawiyah (Radhwiyallahu ‘anhu) …

Read More »

Salaam

Salaam ndi moni wa Chisilamu. Monga momwe Chisilamu chimatanthauza mtendere, moni wa Chisilamu ndi moni wamtendere komanso ofalitsa uthenga wamtendere. Salaam ndi imodzi mwa zochitika zachisilamu zomwe ndi chizindikiro cha Msilamu, ndipo kufunika kwake kwatsindikitsidwa kwambiri mahadith. Olemekezeka Abdullah bin Salaam (Radhwiyallahuanhu) akuti: Mtumiki (madalitso ndi mtendere zikhale pa iye) …

Read More »

Nkhumbo lalikulu la Olemekezeka Saiid bin Zaid (Radhwiya Allaahu ‘anhu) lopereka Moyo Wake Munjira Ya Allah.

Mzinda wa Damasiko utagonjetsedwa ndi Asilamu, Abu Ubaidah (radhwiyallahu ‘anhu) mkulu wa asilikali achisilamu -anasankha Sa’iid bin Zaid (radhwiyallahu ‘anhu) kukhala kazembe wa mzinda wa Damasiko. Pambuyo pake Abu Ubaidah (Radhwiyallahu ‘anhu) adapitilira ndi gulu lake lankhondo kulowera ku Jordan. Atafika ku Yordan, anamanga msasa kumeneko ndi kuyamba kukonzekera zolimbana …

Read More »

Kutonthoza Oferedwa

13. Sizoloredwa kupita ku nyumba ya kafiri yemwe wamwalira kukapepesa mwambo wamaliro uli mkati. Koma akakhala kuti ndi kafiri oyandikana naye nyumba kapena kaafir aliyense amene wataya wachibale wake, mwachitsanzo, mwana, ukhoza kumutonthoza ndi mawu awa: أَخْلَفَ اللّه عَلَيْكَ خَيْرًا مِنْهُوَاَصْلَحَكَ Akhlafa Allahu ‘Alayka Khayran Minhu Wa ‘Aslahaka Allah akupatse …

Read More »

Zida Zikuluzikulu za Dajjaal – Chuma, Akazi ndi Zansangulutso

Dajjaal akadzaonekera padziko, zida zikuluzikulu zomwe adzagwiritse ntchito kusocheretsera munthu ndi chuma, akazi ndi zansangulutso. Allah Ta’ala adzamupatsa mphamvu yochita zozizwitsa kotero kuti onse amene azidzaziona adzakopeka ndi kutengeka ndi fitnah (Mayesero) ake. Allah Ta’ala adzamloleza kugwetsa mvula, kupangitsa nthaka kutulutsa mbewu, ndipo chuma cha m’nthaka chidzamtsatira kulikonse kumene azidzapita. …

Read More »

Hazrat Sa’iid bin Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu) Apirira ku Mavuto Chifukwa Chachisilamu.

Hazrat Umar (radhwiyallahu ‘anhu) – munthu yemwe dzina lake loyera ndi njira yolemekezera chisilamu, ndipo changu cha imaani chinali chotere mpaka lero, patadutsa zaka 1300, anthu osakhulupirira amamuopabe,adali otchuka chifukwa chowazunza Asilamu (iyeyo) asanalowe Chisilamu. Adapitilizanso kufunafuna mipata yomupha Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam). Tsiku lina maquraish adasonkhana. …

Read More »

Kumuzindikiritsa Mwana Kwa Allah

Kulera mwana n’kofunika kwambiri ndipo tingakuyerekezere ndi maziko a nyumba. Ngati maziko a nyumba ali olimba, ndiye kuti nyumbayo idzakhalanso yolimba ndipo idzapirira ku nyengo iliyonse. Mosiyana ndi zimenezi, ngati maziko a nyumbayo ndi ofooka komanso ogwedezekagwedezeka, ndiye kuti ndi kugwedezeka pang’ono, nyumbayo idzagwa. Chimodzimodzinso, kulera mwana ndiko maziko amene …

Read More »

Kutonthoza Oferedwa

7. Nkoloredwa kuyamikira omwalirayo. Komabe, pomutamanda, onetsetsani kuti simukukokomeza kapena kumutamanda pa makharidwe amene panalibe mwa iye. Momwemonso musatengere chikharidwe ndi njira za makafiri pomutamanda. 8. kuchuluka kwa nthawi ya ta’ziyat ndi masiku atatu kuchokera tsiku lomwalira. Pambuyo pa tsiku lachitatu, ndi makruh kupanga ta’ziyat. Komabe, ngati munthu sadathe kubwera …

Read More »