Nthawi ina, Rasullullah (Swallallahu alaihi wasallam) anabwera ku fuko la Bani Zafar (fuko lachi Ansaar). Ali pa mimbar akulankhula nawo, anamuuza Abdullah bin Mas’ood (radhwiyallahu ‘anhu), kuti, “Ndiwerengere Quraan.” Modzichepetsa kwambiri, Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) anauza Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam), “Eh Mtumiki wa Allah, kodi ndikuwerengereni kumachita kuti Quraan …
Read More »Kuwonekera kwa Nkhani Zikuluzikulu Mahdi Asanafike – Zizindikiro za Qiyaamah
Mahdi (radhiyallahu ‘anhu) asanaonekere padziko lapansi, anthu ambiri padziko lonse lapansi adzakhala Akhristu. (Muslim #2898) M’madera ambiri padziko lapansi, Ummah wa Chisilamu udzakhala ukuvutika ndipo udzazunzidwa ndi kuvutitsidwa ndi makafiri. Nkhondo zambiri zidzabuka ndipo Asilamu padziko lonse lapansi adzakhala akuyembekezera mwachidwi kubwera kwa Mahdi (radhiyallahu ‘anhu) kuti awathandize. Panthawiyo, Sufyaani …
Read More »Sunnats Ndi Aadaab Pa Kumwa 1
1)Musanamwe, Nenani dzina la Allah powerenga بِسْمِ الله M’dzina la Allah. 2) Imwani ndi dzanja lamanja. Olemekezeka Ibnu Umar radhwiyallah anhuma akunena kuti Rasulullah adati, “Aliyense wa inu akamayamba kudya, ayenera kudyera dzanja lake lamanja, ndipo akamamwa, ayenera kumwera dzanja lake lamanja, pakuti Shaitaan amadya ndi dzanja lake lamanzere ndi …
Read More »Chitsimikizo Cha Sayyiduna Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) Pa Mawu a Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam)
Ulendo wina, nthawi ya khilaafat yake, Sayyiduna Uthmaan (radhwiyallhu ‘anhu) anabwera kudzacheza ndi Olemekezeka Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu). Apa ndikuti Abdullah bin Masood (radhwiyallahu ‘anhu) akudwala matenda ake omaliza. Sayyiduna Uthman (radhwiyallahu ‘anhu) anamufunsa kuti, “Ndi vuto lanji lomwe likukusautsa?” Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) anayankha kuti, “Chomwe chikundisautsa …
Read More »Kumwa
Pali ma sunnah ndi ma adaab ambiri okhudzana ndi kumwa. Ma sunnah ndi ma adaab ena amakhudzana ndi madua osiyanasiyana omwe alamulidwa kuti awerengedwe usanayambe kumwa, pamene ukumwa komanso utamaliza. Ma sunnah ndi ma adaab ena amakhudzana ndi momwe munthu angamwere. Kupatula izi, pali ma sunnah ndi ma adaab omwe …
Read More »Hazrat Abdullah ibn Mas’uud (radhiyallahu anhu) Kuwerenga Qur’aan Majeed mokweza mawu pamaso pa Aquraish
Hazrat Abdullah ibn Mas’uud (radhiyallahu anhu) adali munthu oyamba kuwerenga Qur’aan Majeed mokweza mawu ku Makkah Mukarramah Aquraish asanalowe Chisilamu. Tsiku lina, maSwahaabah (radhiyallahu anhum) anasonkhana nati, “Ndikulumbira mwa Allah, Aquraish sanamvepo wina akuwerenga Qur’aan mokweza mawu pamaso pawo, ndiye ndani pakati pathu amene ali okonzeka kupita kukawerenga Qur’aan mokweza …
Read More »Moyo Wa Nabi Issah Alaihis Salaam Akadzabweranso Padziko Lapansi Ndi Kuchuluka Kwa Madalitso Ndi Chitetezo Mnthawi Yake
Nabi Isa (‘alaihis salaam) akadzabwerera padziko lapansi, Mahdi (radhiyallahu ‘anhu) adzakhala mtsogoleri otsogolera Asilamu. Mahdi (radhiyallahu ‘anhu) adzauza Nabi Isa (‘alaihis salaam) kuti atsogolere Asilamu, popeza iye ndi Nabi wa Allah Ta‘ala. (Ibnu Hibbaan #6812, Fitan li-Nu’aim #1028) Asilikali achisilamu, motsogozedwa ndi Nabi Isa (‘alaihis salaam), adzamenyana ndi Dajjaal komanso …
Read More »Ma Dua Onena Ukamaliza Kudya 2
Dua 6 اَلْحَمْدُ للهِ الَّذي أَطْعَمَ وَلَا يُطْعَمُ مَنَّ عَلَيْنَا فَهَدَانَا وَأَطْعَمَنَا وَسَقَانَا وَكُلُّ بَلاَءٍ حَسَنٍ الحَمْدُ لِلهِ الَّذِي أَطْعَمَ مِنَ الطَّعَامِ وَسَقَى مِنَ الشُّرْبِ وَكَسَا مِنَ الْعُرۡيِ وَهَدٰى مِنَ الضًّلاَلَةِ وَبَصَّرَ مِنَ العَمٰي وَفَصَّلَ عَلٰى كَثِيرٍ مِمَّنْ خَلَقَ تَفْضِيْلاً ألْحَمْدُ للهِ رَبِّ الْعَالَمِين Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene …
Read More »Kulimba Mtima kwa Hazrat Abdullah bin Mas’uud (Radhiyallahu ‘anhu)
Pankhondo ya Hunain, Asilamu adagonjetsedwa kwakanthawi kochepa. Munthawi yovutayi, Hazrat Abdullah bin Mas’uud (Radhwiyallahu ‘anhu) adali m’gulu la ma swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) amene adapirirabe ndikukhala limodzi Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam). Hazrat Abdullah bin Mas’ood (radhwiyallahu ‘anhu) akufotokoza kuti: “Ndinali ndi Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) tsiku la …
Read More »Ma Dua Onena Ukamaliza Kudya
Dua Yoyamba اَلْحَمْدُ لِله الَّذِي أَطْعَمَنَا وَسَقَانَا وَجَعَلَنَا مُسْلِمِينَ Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene watipatsa chakudya ndi chakumwa ndi kutipanga kukhala Asilamu. Dua Yachiwiri الْحَمْدُ لِلَّهِ الَّذِي أَطْعَمَنِيْ هَذَا الطَّعَامَ وَرَزَقَنِيْهِ مِنْ غَيْرِ حَوْلٍ مِّنّّي وَلاَ قُوَّةٍ Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah amene wandipatsa chakudya ichi kuti ndidye, ndipo …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu