6. Pangani ma dua komanso azkaar musanagone; اللَّهُمَّ بِاسْمِكَ أَمُوْتُ وَأَحْيٰ O, Allah Talaa mdzina Lanu ndikufa komanso ndiuka 7. Gonerani kumanja ndikuika dzanja lanu lamanja pansi pa tsaya lanu lakumanja. Bibi Hafsah (radiyallahu anha) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) akafuna kugona, ankaika dzanja lake lamanja pansi pa tsaya …
Read More »Munthu Olungama Kwambiri – Fudhail Bin Iyaaz Rahimahullah
Fudhail bun Iyaaz (Rahimahullah) aDali Muhaddith olemekezeka komanso oyera mtima wa m’nthawi yake. Allah Talaa adamdalitsa ndi ulemelero wapamwamba kwambiri mu Hadith kotero kuti ambiri mwa ma Muhadith otsogola, monga Abdullah bin Mubaarak, Sufyaan bun Uyainah ndi Imaam Shaafi’e (Rahimahullah) adafotokoza Hadith kuchokera kwa iye. Zanenedwa kuti Fudhail (Rahimahullah) asanadalitsidwe …
Read More »Rasulullah (Swallallahu ‘alaihi wasallam) Amuitana Abdullah bin Mas’ud (radhwiyallahu ‘anhu) ku Moyo Osatha
Salamah bin Tammaam (rahimahullah) akufotokoza kuti: Masiku angapo Abdullah bin Mas’ud (radhiyallahu ‘anhu) asanamwalire, munthu wina adabwera kudzakumana naye. Atakumana naye, munthuyo anamuuza kuti, “Oh Ibnu Mas’ud! Usiku watha, ndinakulota. M’maloto, ndinamuona Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) atakhala pa guwa pomwe iwe unali pansi pake. “Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) anakulankhula nanu …
Read More »Sunnati Ndi Adaab 1
1. Mukamaliza Swala ya Esha, musakhale kumacheza nkhani zopanda pake mmalo mwake yesetsani kugona mwachangu kuti mudzukire Tahajjud komanso Swala ya Fajr mnthawi yake. Komabe, ngati pali chifukwa chomveka, monga kukambirana ndikuchita za Dini mutha, kukambirana za malamulo a Dini mashwarah ofunikira, ndi zina zotero. ndiye kuti mudzaloredwa kuchita nawo …
Read More »Osataya Chiyembekezo Mu Kusinthika Kwa Munthu Aliyense
Abdullah bin Maslamah Q’anabi (rahimahullah) anali m’gulu la ma Muhadditheen otsogola mu nthawi yake. Iye anali mtsogoleri wa ma Muhadditheen ambiri otchuka, ngati Imaam Bukhaari, Imaam Muslim ndi Imaam Abu Dawood (rahimahullah) Zikunenedwa kuti pachiyambi cha moyo wake, ankacheza ndi anthu oipa ndipo ankamwa mowa. Komabe, atakumana ndi Muhaddith …
Read More »Tafseer Ya Surah Abas
بِسْمِ اللَّهِ الرَّحْمَٰنِ الرَّحِيمِ عَبَسَ وَتَوَلَّىٰ ﴿١﴾ أَن جَاءَهُ الْأَعْمَىٰ ﴿٢﴾ وَمَا يُدْرِيكَ لَعَلَّهُ يَزَّكَّىٰ ﴿٣﴾ أَوْ يَذَّكَّرُ فَتَنفَعَهُ الذِّكْرَىٰ ﴿٤﴾ أَمَّا مَنِ اسْتَغْنَىٰ ﴿٥﴾ فَأَنتَ لَهُ تَصَدَّىٰ ﴿٦﴾ وَمَا عَلَيْكَ أَلَّا يَزَّكَّىٰ ﴿٧﴾ وَأَمَّا مَن جَاءَكَ يَسْعَىٰ ﴿٨﴾ وَهُوَ يَخْشَىٰ ﴿٩﴾ فَأَنتَ عَنْهُ تَلَهَّىٰ ﴿١٠﴾ كَلَّا إِنَّهَا تَذْكِرَةٌ ﴿١١﴾ فَمَن شَاءَ ذَكَرَهُ ﴿١٢﴾ فِي صُحُفٍ مُّكَرَّمَةٍ ﴿١٣﴾ مَّرْفُوعَةٍ مُّطَهَّرَةٍ Iye (Mtumiki [swallallahu alaihi wasallam]) anachita tsinya natembenukira kumbali chifukwa chobwera kwa iye munthu wakhungu! Ndipo …
Read More »Kusamalitsa kwakukulu Kwa Sayyiduna Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) Potulutsa mahadith a Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam)
Ole.wkezeka ‘Amr bin Maimoon (rahimahullah) adafotokoza za kusamalitsa kwakukulu kwa Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) pamene ankatulutsa mahaadith kuchokera kwa Rasulullah (ssallallahu alaihi wasallam). Adanena kuti, “Nthawi ina, Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) atayamba kunena Hadith yochokera kwa Rasulullah (sallallahu alaihi wasallam), adagwidwa ndi mantha ndi nkhawa kotero kuti madontho …
Read More »Gulu Lankhondo Lokhala ndi Mbendera Zakuda Lochokera ku Khurasaan
Pambuyo poti Mahdi waonekera pakati pa anthu ndipo nkhani ya kuonekera kwake yayamba kufalikira padziko lonse lapansi, gulu lankhondo lokhala ndi mbendera zakuda lidzachoka ku Khurasaan kupita ku Makkah Mukarramah ndikukhalira limodzi ndi Mahdi. Rasulullah (Swallallahu ‘alaihi wasallam) adalimbikitsa ummah kuti udzakhale ndi gulu lankhondo limeneli pobwera kwa Mahdi. Rasulullah …
Read More »Kugona
Tulo ndi chimodzi mwa zinthu zofunikira kwambiri kwa munthu aliyense, monga mmene kudya ndi kumwa zilili zofunikira kwambiri. Allah Talaa akutchula za ubwino waukulu wa tulo mu Qur’aan Majiid ponena kuti: Ndipo tidakupangirani tulo kukhala mpumulo. M’ndime ina Allah Talaa akuti: Iye ndi Yemwe adakupangirani usiku kukhala chovala (chokuphimbani ndi …
Read More »Hazrat Abdullah bin Mas’uud (radhiyallahu ‘anhu) ndi Izindikiri wake a Quraan Majiid
Shaqiiq bin Salamah (rahimahullah), ophunzira wa Abdullah bin Mas’uud (radhiyallahu ‘anhu), akunena kuti nthawi ina yake, Abdullah bin Mas’uud (radhiyallahu ‘anhu) adapereka khutbah. Mu khutbahmo adati, “Ndikulumbira qasam mwa Allah! Ndinaphinzira ma surah oposa makumi asanu ndi awiri a Quraan Kariim mwachindunji kuchokera kwa Rasulullah (sallallahu alaihi wasallam). Ndikulumbira m’dzina …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu