Mtumiki (Swallallahu ‘alaihi wasallam) asankha Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) kukhala Bwanamkubwa wa Yemen

Rasulullah (Swallallahu ‘alaihi wasallam) pomutumiza Mu’aaz (radhwiyallahu ‘anhu) ku Yemen, adamufunsa kuti, “Ndi njira yanji yomwe udzatsatire ukamakapereka chigamulo pa nkhani za Asilamu?” Mu’aaz (Radhwiyallahu ‘anhu) adayankha kuti: “Ndidzagwiritsa ntchito Qur’aan.” Kenako Nabi (Swallallahu ‘alaihi wasallam) adamufunsa kuti: “Ngati lamulo silikupezeka mu Qur’aan udzatani?” Iye adayankha kuti, “Ndidzagwiritsa nctchito mahaadith …

Read More »

Kutuluka kwa Dajjaal ndi Ma Fitnah Ake Osiyanasiyana

Dajjaal akadzaonekera padziko lapansi, adzayamba kutulukira ndi kum’mawa kwa dziko, pakati pa Syria ndi Iraq. Pambuyo pake, adzapita ku Isfahaan komwe Ayuda 70,000 adzakhale naye limodzi. (Muslim #2944) Adzayenda padziko lonse lapansi, ndipo kulikonse komwe akupita, adzabweretsa fitnah yaikulu komanso ziphuphu zambiri. Malo awiri okha omwe sadzatha kulowamo ndi Makkah …

Read More »

Kuyamika Pa Mdalitso Okhala Ndi Moyo

Dawuud bin Dinaar anali Imaam wamkulu pankhani ya Hadith komanso mphunzitsi wa ma Muhadditheen otchuka, monga Imaam shu’bah (rahimahullah) ndi Imaam Wakii (rahimahullah). Mkatikati mwa moyo wake kunadzabuka mliri ku Khuraasaan kumene ankakhala omwe udakhudza anthu ndipo ambiri adataya miyoyo yawo. Dawuud bin Dinaar (rahimahullah) anali m’gulu la omwe adagwidwa …

Read More »

Kudziwa Kwambiri Dini kwa Muaaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu)

Abu Muslim Khowlaani (rahimahullah) akufotokoza kuti: “Ndinalowa mumzikiti wa Hims ndipo ndinaona gulu la anthu. Pakati pawo panali anzake makumi atatu ndi awiri a Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) omwe ankakambirana za mahadith kuchokera kwa Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam). Munkumanowu munali mnyamata, amene maso ake anali atapakidwa surma ndipo mano ake …

Read More »

Sunnati Ndi Adaab 3

12. Ngati mungadzukire pakati pa usiku, werengani dua yotsatirayi ya masnun ndipo pambuyo pake mutha kupempha kwa Allah Talaa. Insha Allah, dua yanu idzalandiridwa. لَا إِلٰهَ إِلَّا اللهُ وَحْدَهُ لَا شَرِيْكَ لَهُ لَهُ الْمُلْكُ وَلَهُ الْحَمْدُ وَهُوَ عَلٰى كُلِّ شَيْءٍ قَدِيْرْ اَلْحَمْدُ لِلّٰهِ وَسُبْحَانَ اللهِ وَلَا إِلٰهَ إِلَّا اللهُ وَاللهُ …

Read More »

Imaam Ahmad bin Hambal (rahimahulla) Kupindura kuchoka kwa Bishr Haafi (rahimahulla)

Nkhani yotsatirayi ikuunikira kumvetsetsa kwakuya kwa dini ndi ma’rifat (kuzindikirika) ya Allah Talaa zomwe Allah Talaa adamudalitsa nazo Bishr Haafi (rahimahulla) zomwe zidachititsa kuti mpaka Imam Ahmad (rahimahulla) amutsanzire: M’nthawi ya Imaam Ahmad bin Hambal (rahimahulla) kunali dotolo wina yemwe ankatchedwa kuti Abdur Rahmaan At-Tabeeb. Ankathandiza Imaam Ahmad bin Hambal …

Read More »

Chikondi cha Rasulullah (Sallallahu ‘alaihi wasallam) kwa Sayyiduna Muaaz bin Jabal (radhiwyallahu ‘anhu)

Sayyiduna Muaaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) akunena kuti nthawi ina, Nabi (Swallallahu alaihi wasallam) anagwira dzanja langa nati kwa ine, “O Muaaz!”, ndipo ine ndinayankha kuti, “Ndili pano kuti ndikutumikireni.” Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) kenako anandiuza kuti, “Ndithudi, ndimakukonda (chifukwa cha Allah Ta’ala).” Muaaz bin Jabal (Radhwiyallahu ‘anhu) anayankha kuti, …

Read More »

Kupereka kwa Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu)

Nthawi ina,Olemekezeka Umar (radhwiyallahu ‘anhu) anatumiza ndalama zagolide mazana anayi kwa Abu ‘Ubaidah bin Jarraah (radhwiyallahu ‘anhu) ndipo analamula mthumwiyi kuti ikadikire pang’ono kuti aone zomwe achite nacho chumacho. Olemekezeka Abu Ubaydah (radhwiyallahu ‘anhu) atalandira ndalamazo, anati, “Allah amuchitire chifundo (kunena Umar).” Kenako anauza kapolo wake wamkazi kuti, “Tenga ndalama …

Read More »

Nkhondo Yaikulu ndi Kugonjetsedwa kwa Istanbul

Mahdi atabwera, Allah Ta‘ala adzawapatsa Asilamu uysogoleri ndi mphamvu padziko lonse lapansi. Akristu adzazindikira kuti Asilamu akupeza thandizo ndipo akukula mphamvu tsiku ndi tsiku. Kenako adzakonza gulu lankhondo lalikulu kuti amenyane ndi Mahdi ndi Asilamu. Zanenedwa mu Hadith kuti Akristu ochokera m’maiko onse adzasonkhanitsa asilikali awo ndikukonzekera kumenyana ndi Asilamu. …

Read More »