Zotsatira Za Kuipa Kwa Vinyo. Mankhwala Ozunguza Ubongo Ndi Zoledzeretsa

Tikayerekeza dini ya Chisilamu ndi zipembedzo zakale, timapeza kuti Chisilamu sichinangolongosora machimo ndi ntchito zoipa kuti ndi haraam, komanso chinafotokoza njira zomwe zimatsogolera ku uchimo ndi zoipa ngati haraam. Izi zidachitika kuti zimuteteze munthu kuti asagwere mu uchimo. Taganizirani chitsanzo cha mowa chomwe chinali choloredwa m’zipembedzo zakale, koma chanenedwa kuti …

Read More »

Uphungu wa Abdullah bin Abbaas (radhiyallahu ‘anhuma)

Wahab bin Munabbih (rahimahullah) akunena kuti: Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhiyallahu ‘anhuma) atasanduka wakhungu (ku ukalamba wake), ndidamutsogolera ku Haram Sharif ku Makkah Mukarramah, komwe anamva gulu la anthu likukangana pakati pawo. Anandipempha kuti ndimulondolere kwa iwo. Atafika kwa iwo, anawalonjera ndi mawu onena kuti “Assalaamu Alaikum”. Anamupempha kuti akhale …

Read More »

kuzindikira kwakukulu kwa Abdullah bin Abbaas (radhiwyallahu ‘anhuma)

Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhwiyallahu ‘anhuma) akuti: Mtumiki wa Allah (swallallahu ‘alaihi wasallam) atamwalira, ndinauza mnzanga wina wachi Ansaari kuti, “Bwera, tiye tipite tikaphunzire (Dini) kuchokera kwa Ma Sahaabah (radhwiyallahu ‘anhum), pomwe ambiri a iwo akadalipo pakati pathu.” Anandiyankha kuti, “Iwe Ibnu Abbaas! Ndikulumbira mwa Allah, ndikudabwa kuti ukuganiza kuti …

Read More »

Kachitidwe ka Mu’aaz (radhiyallahu ‘anhu) Kuwerenga Quraan Majeed pa Tahajjud

Mtumiki (swallallahu ‘alaihi wasallam) anatumiza Mu’aaz (radhwiyallahu ‘anhu) kuti akalamulire gawo lina la Yemen, ndipo Abu Musa Ash’ari (radhwiyalllahu ‘anhu) akalamulire gawo lina. Mtumiki (swallallahu ‘alaihi wasallam) anawalankhula ndipo anawapatsa uphungu otsatirawu asanawatumize. Anawauza kuti, “Fewetsani zinthu (kwa anthu), ndipo musawakhwimitsire. Perekani uthenga wabwino (kwa anthu), ndipo musawathamangitse (ku dini).” …

Read More »

Zinthu Zomwe Zimachititsa Kuti Mdalitso Wa Allah Uchoke

Kuipa Kojambula Zithunzi Tiku lina Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) kulibe ali koyenda, Bibi Aaishah adapachika katani yokhala ndi zithunzi za zinthu zamoyo pakhomo. Nthawiyo Sayyidah Aaishah (radhwiyallahu anha) sankadziwa kuti zithunzi za zinthu zamoyo zinali zoletsedwa. Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) atafika kunyumba kwake ndipo maso ake anagwera pa katanilo anakwiya …

Read More »

Ubale Wapafupi Umene Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) Anasangalala Nawo Ndi Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam)

Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) akunena kuti, “Nthawi ina, ndinali nditakhala kumbuyo kwa Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) pa bulu pamene naye analinso pomwepo. Panalibe chilichonse pakati pa ine ndi Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kupatula thabwa la chokhalira (chomwe chimalekanitsa okwera ndi munthu amene wakhala kumbuyo kwake). “Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) …

Read More »

Madua Ndi Azkaar Ogonera

Dua 1 اَللّٰهُمَّ بِاسْمِكَ أَمُوْتُ وَأَحْيٰى Eh Allah! Talaa mdzina Lanu ndidzafa ndikukhala ndi moyo. Dua 2 اَللّٰهُمَّ قِنِيْ عَذَابَكَ يَوْمَ تَبْعَثُ عِبَادَكَ Eh, Allah! ndipulumutseni ku chilango Chanu tsiku limene Mudzaukitse akapolo Anu (m’manda). Dziwani: Mtumiki (sallahu alayhi wasalam) ankawerenga dua iyi. Duwa 3 اَلْحَمْدُ لِلّٰهِ الَّذِيْ أَطْعَمَنَا وَسَقَانَا …

Read More »

Malangizo Otsanzikirana a Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kwa Mu’aaz (radhwiyallahu ‘anhu) pamene ankamutumiza ku Yemen

Pamene Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) ankatumiza Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) ku Yemen kuti akaphunzitse anthu dini ndikuwalamulira, posiyana naye, Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) ankayenda naye mpaka kunja kwa mzinda wa Madinah Munawwarah pamene ankamupatsa uphungu osiyanirana. Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) anamulamula kuti achite zinthu zina zabwino, ndipo anamulamula kuti …

Read More »

Kumapeto Kwa Moyo Wa Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) Padziko Lapansi

Mtumiki (swallallahu ‘alayhi wasallam) adati, “Munthu amene amamwalira ndi mliri, amakhala wamwalira imfa ya shahid. Mu khilaafat ya Umar (radhwiyallahu ‘anhu), mliri wa Amwaas unakhudza Shaam m’chaka cha 17 pambuyo pa Hijrah. Mu mliriwu Abu Ubaidah (radhwiyallahu ‘anhu), mtsogoleri wa Asilamu ku Shaam, anakhudzidwa nawonso ndipo pambuyo pake anamwalira. Asanamwalire, …

Read More »