Daily Archives: July 29, 2024

Kulimba Mtima kwa Zubair (Radhiyallahu ‘anhu)

Patsiku la (nkhondo) ya Yarmuuk, ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) adati kwa Zubair (Radhiyallahu ‘anhu): “Bwanji siukupita ndi kukamenyana ndi adani, ndipo ife tidzakutsatira pokalimbana ndi adani.?” Zubair (Radhwiya Allahu ‘anhu) adayankha: “Ndikudziwa kuti ngati ndingapite anthu inu simungagwirizane nane.” Ma Swahaabah (Radhiyallahu ‘anhum) adati: “Ayi, ife tikugwirizana nawe ndipo tikutsatira.” …

Read More »