Daily Archives: August 19, 2024

Khumbo la Umar (Radhwiyallahu ‘anhu) kudalitsidwa ndi Chipinda Chodzaza ndi Anthu monga Abu Ubaidah (radhiyallahu ‘anhu)

Umar (Radhwiyallahu ‘anhu) nthawi ina anakhala pansi ndi gulu la maswahabah pamene iye analankhula nawo ndipo kenako anafunsa funso lonena kuti, “Tandiuzani chimene anthu inu mukulakalaka” Munthu wina adati: “Chokhumba chomwe ndili nacho ndikuti chipinda chonsechi chitadzadza ndi ma dirham (ndalama zasiliva) ndikuti ndiwononge zonsezo panjira ya Allah Ta’ala.” Umar …

Read More »