Daily Archives: August 22, 2024

Kodi Amaanah Imatanthauza Chiyani?

Amaanah imatanthauza kuti munthu akhale olingalira za tsiku lachiweruzo pamene adzaime pamaso pa Allah pankhani ya maudindo amene munthu ali nawo kwa Allah ndi akapolo a Allah. Limeneri ndi khalidwe labwino kwambiri kotero kuti ndi khomo lopezera zabwino zosawerengeka za uzimu ndi thupi zochoka kwa Allah. Ubwino wa amaanah umapanga …

Read More »