Daily Archives: February 3, 2025

Mantha a Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) kuyankha mlandu ngakhale adawonongera chuma pa ntchito ya Dini.

Shu’bah (Rahimahullah) akuti: Nthawi ina Abdur Rahman bun Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) ankasala kudya ndipo nthawi ya iftaar, chakudya chinabweretsedwa kwa iye. Ataona chakudyacho, Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) adati: “Hamzah (Radhwiyallahu ‘anhu) adaphedwa chifukwa cha chikhulupiriro ndipo sitinapeze nsalu yokwanira sanda yake, ndipo anali wabwino kuposa ine. Mus’ab bin …

Read More »