Daily Archives: February 18, 2025

Abdur Rahmaan bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) agwiritsa ntchito Chuma chake pa nkhondo ya Tabuk.

Pamene Allah Ta’ala ankamulamula Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) kuti anyamuke ulendo wa ku Tabuk, ma Swahaabah ambiri adalibe kalikonse panthawiyo zoti athandizikirw kuyende ulendo wautali ndi wotopetsa, makamaka pamene ankayembekezera kukumana ndi gulu lankhondo lachiroma pankhondo yomwe inali ndi zida zokwanira komanso adalipo ambiri. Choncho pofuna kusonkhanitsa pamodzi ndi …

Read More »