M’chaka cha chisanu ndi chimodzi chioangireni Hijrah, m’mwezi wa Sha’baan, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adalankhula ndi Abdur Rahmaan bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) nati kwa iye: “Konzekeretsa ulendo wako, popeza ndikufuna ndikutumize ku ulendo, mwina lero kapena mawa, Insha Allah. M’mawa mwake, Abdur Rahmaan bun Auf (Radhiyallahu ‘anhu) …
Read More »