6. Pangani ma dua komanso azkaar musanagone; اللَّهُمَّ بِاسْمِكَ أَمُوْتُ وَأَحْيٰ O, Allah Talaa mdzina Lanu ndikufa komanso ndiuka 7. Gonerani kumanja ndikuika dzanja lanu lamanja pansi pa tsaya lanu lakumanja. Bibi Hafsah (radiyallahu anha) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) akafuna kugona, ankaika dzanja lake lamanja pansi pa tsaya …
Read More »Sunnati Ndi Adaab 1
1. Mukamaliza Swala ya Esha, musakhale kumacheza nkhani zopanda pake mmalo mwake yesetsani kugona mwachangu kuti mudzukire Tahajjud komanso Swala ya Fajr mnthawi yake. Komabe, ngati pali chifukwa chomveka, monga kukambirana ndikuchita za Dini mutha, kukambirana za malamulo a Dini mashwarah ofunikira, ndi zina zotero. ndiye kuti mudzaloredwa kuchita nawo …
Read More »Kugona
Tulo ndi chimodzi mwa zinthu zofunikira kwambiri kwa munthu aliyense, monga mmene kudya ndi kumwa zilili zofunikira kwambiri. Allah Talaa akutchula za ubwino waukulu wa tulo mu Qur’aan Majiid ponena kuti: Ndipo tidakupangirani tulo kukhala mpumulo. M’ndime ina Allah Talaa akuti: Iye ndi Yemwe adakupangirani usiku kukhala chovala (chokuphimbani ndi …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu