Kugona

Kugona

Tulo ndi chimodzi mwa zinthu zofunikira kwambiri kwa munthu aliyense, monga mmene kudya ndi kumwa zilili zofunikira kwambiri. Allah Talaa akutchula za ubwino waukulu wa tulo mu Qur’aan Majiid ponena kuti: Ndipo tidakupangirani tulo kukhala mpumulo. M’ndime ina Allah Talaa akuti: Iye ndi Yemwe adakupangirani usiku kukhala chovala (chokuphimbani ndi …

Read More »