Daily Archives: October 9, 2024

Ntendere Waukulu Wa Allah Pa Akapolo Ndi Kukhala Makolo

Ena mwa madaritso aukuluakulu a Mulungu pa munthu, ndi mdaritso okhala ndi makolo. Mwayi okhalandi makolo ndi mdaritso ofunika kwambiri ndipo ulibe mlowa m’malo komanso umaperekedwa kwa munthu kamodzi kokha m’moyo wake. Monga momwe chisomo cha kukhala ndi moyo chimaperekedwa kamodzi kokha kwa munthu, ndipo chikatha sichidzabwereranso, momwemonso chisomo chokhala …

Read More »