Daily Archives: October 14, 2024

Kuopa Allah Taala

Qataadah (Rahimahullah) akusimba kuti Olemekezeka Abu Ubaidah (Radhwiyallahu ‘anhu) ankati, (chifukwa choopa kudzaima pamaso pa Allah Ta’ala pa tsiku la Qiyamah ndi kuwerengetsedwa ntchito zake. وددت أني كنت كبشا، فيذبحني أهلي، فيأكلون لحمي، ويحسون مرقي. “Ndikulakalaka ndikadakhala nkhosa. Ondipha akadandipha, akanadya nyama yanga ndikumwa nsuzi wanga. (Siyaru Aa’laamin Nubalaa 3/14) …

Read More »