Daily Archives: December 30, 2024

Mlamu wa Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam)

Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) adakwatira akazi okwana anayi. Aliyense mwa akazi ake anayi anali pachibale ndi m’modzi mwa akazi olemekezeka a Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi waaalihi wasallam). Ndichifukwa chake Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adamuuza kuti: “(Ndiwe) mlamu wanga padziko lapansi ndi tsiku lotsiriza (kutanthauza kuti udzakhalanso mlamu wanga …

Read More »