Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) adakwatira akazi okwana anayi. Aliyense mwa akazi ake anayi anali pachibale ndi m’modzi mwa akazi olemekezeka a Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi waaalihi wasallam). Ndichifukwa chake Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adamuuza kuti: “(Ndiwe) mlamu wanga padziko lapansi ndi tsiku lotsiriza (kutanthauza kuti udzakhalanso mlamu wanga …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu