20. Musatemberere ana anu pamene mukupempha pa Swalah kapena nthawi ina iliyonse. Ndizotheka kuti temberero lanu litha kukumana ndi nthawi yomwe ma dua amayankhidwa. Olemekezeka Jaabir (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Musadzitemberere nokha, ana anu, akapolo anu, kapena chuma chanu.Temberero lanu likhoza kukumana ndi nthawi (yoyankhidwa) …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu