Mkazi wa Talhah (Radhwiyallahu ‘anha), Su’da bint ‘Awf al-Muriyyah anakambapo izi zokhudza mwamuna wake Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu): “Tsiku lina Talha analowa m’nyumba ali okhumudwa. Chavuta ndi chiyani? Kodi ndalakwitsa penapake mchifukwa ndikuwona kuti mukuonetsa kukhumudwa? Chonde ndiuzeni kuti ndithe kuchotsa kukhumudwa kwanu. Iye adayankha, “Ayi, siunandilakwire chilichonse, ndipo ndithudi, ndiwe …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu