M’mahadithi olemekezeka, Olekezeka Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adatsimikizira ummah za Maonekedwe a Dajjaal a umunthu. Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kufotokoza za Dajjaal m’maonekedwe a munthu zikuonetsa kuti Dajjaal ndi munthu. Pa chifukwa chimenechi, chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah ndi chakuti Dajjaal ndi munthu, ndipo adzabwera pa dziko lapansi nthawi …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu