Naufal bin lyaas al Huzali (rahimahullah) adati: ‘Tikakhala pamodzi ndi Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu), ndi kukhala naye chifupi kodabwitsa kusangalatsirenji. Tsiku lina, anatitengera kunyumba kwake kuti tikadye, Titakhala pansi kuti tidye ndipo mbale ya chakudya ya nyama ndi mkate inaperekedwa pamaso pathu, iye adayamba kulira. Tidamufunsa: “Nchiyani chikukupangitsa …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu