1. Werengani Surah Dukhaan Lachinayi usiku. Olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallah anhu) akunena kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati, munthu amene amawerenga Surah Haa-meem Ad-Dukhaan usiku wa Jumu’ah ( Lachinayi usiku), machimo ake adzakhululukidwa.” 2. Sambani (ghusl) Lachisanu. Munthu amene amasamba Lachisanu, machimo ake ang’onoang’ono amakhululukidwa. Olemekezeka Abu Bakr Siddeeg (radhwiyallahj …
Read More »Olemekezeka Abu Zar (Radhwiyallahu ‘anhu) Kulemekeza Alendo
‘Isa bin ‘Umailah (Rahimahullah) akufotokoza za munthu wina amene adawona khalidwe la Abu Zar (Radhwiyallahu ‘anhu) kwa anansi ake ndi alendo. Akunena kuti: “Nthawi iliyonse Abu Zar radhwiyallahu anhu akamakama mkaka wa mbuzi zake, poyamba ankagaira mkakawu anthu oyandikana nawo nyunba ndi alendo ake kuti ayambe amwa iwowo kenako ankamwa …
Read More »Momwe Mungadzipulumutsire ku Fitnah (Mayesero)za Dajjaal
M’mahadith odalitsika, Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adaupatsa ummah mankhwala odzitetezera ku ma Fitna a nthawi zonse komanso Mayesero a Dajjaal. Zanenedwa kuti Olemekezeka Uqbah bin Aamir (radhwiyallahu ‘anhu) nthawi ina adamufunsa Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam), “Oh Rasul wa Allah (swallallahu ‘alaihi wasallam)! Kodi njira yopezera chipulumutso ndi iti (kuchokera ku …
Read More »Chilungamo Cha Sheikh Abdul Qadir Jeelani (rahimahullah)
Sheikh Abdul Qaadir Jeelani (rahimahullah) anali Aalim ndi Wali wa Allah Ta‘ala yemwe anakhalapo m’zaka za mma 600 A.H. Allah Ta‘ala adamudalitsa ndi kulandiridwa kwakukulu kotero kuti anthu ambiri adasintha miyoyo yawo ndi iye. Khalidwe limodzi lodziwika bwino lomwe lidawonekera m’moyo wake linali chilungamo (kuyankhula chilungamo). Pansipa pali nkhani yomwe …
Read More »Kulowa Chisilamu kwa Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu)
Khalidwe lake Asanalowe Chisilamu: Asanalowe Chisilamu, Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu) anali chigawenga. Anali olimba mtima kwambiri kotero kuti popanda kuthandizidwa ndi anzake ena, ankakwanitsa yekha kubera anthu ndikuwachita uchifwamba. Nthawi zina, ankaukira anthu apaulendo atakwera pahatchi, ndipo nthawi zina, ankaukira akuyenda pansi. (Siyar A’laam min Nubalaa 3/373) Pambuyo pake, anasiya …
Read More »Bilaal (Radhwiyallahu ‘anhu) Kubwerera ku Madina Munawwarah
́Allaamah Zurqaani (Rahimahullah) wapereka nkhani iyi kuchokera kwa Haafiz ibn ‘Asaakir (rahimahullah) ndi mndandanda wamphamvu wa osimba nkhani: Atamwalira Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam), zinali zovuta kwa olemekezeka Bilaal (radhwiyallahu ‘anhu) kupitiriza kukhala ku Madinah Munawwarah cha okondeka wake kwambiri Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) ndi …
Read More »Ubwino wa Jumuah
Kukhululukidwa Kwa Machimo kudzera mukuswali Jumuah Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Machimo omwe achitika pakati pa Jumu’ah ziwiri, ngati sali machimo akuluakulu, Allah amakhululuka. Tsiku Lopatulika kwa Okhulupirira Ibnu Abbaas (radhwiyallahu anhuma) adanena kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Tsiku ili (tsiku la Jumu’ah) …
Read More »Dua ya Bilaal (Radhwiyallahu ‘anhu) kuwapemphera chiongoko ma Quraish.
Olemekezeka ‘Urwah bun Zubair (rahimahullah) anasimba kuti mkazi wina wa m’banja la Banu Najjaar (yemwe ndi Nawwaar bint Maalik, mayi ake a Zaid bin Thaabit (radhwiyallahu ‘anhuma)) adati: “Nyumba yanga inali pamalo okwera ndipo inali imodzi mwa nyumba zapamwamba za Mus. “Bilaal (Radhwiya Allaahu ‘anhu) ankaitana azaan ya Fajr kuchokera …
Read More »Jumuah
Tsiku la Jumu’ah ndi lofunikira kwambiri mu Chisilamu. Izi ndi zina mwa zabwino zazikulu za Allah pa Ummah uwu ndipo ndichinthu chodziwika bwino m’Chisilamu. Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) adati: “Tsiku la Jumu’ah ndi sayyidul ayyaam (lomwe ndi mtsogoleri wa masiku onse), ndi tsiku lalikulu kwambiri (kuchokera m’masiku a msabata) pamaso …
Read More »Olemekezeka Bilaal (Radhwiya Allaahu ‘anhu) Ayang’anira ndi Kusunga Mkondo wa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam)
Mfumu yaku Abysinia (Najaashi (rahimahullah)) nthawi ina inatumiza mikondo itatu kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) ngati mphatso. Atalandira mikondo itatu ija, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) adapereka mkondo umodzi kwa Ali (radhwiyallahu ‘anhu), adapereka mkondo wachiwiri kwa Umar (Radhwiyallahu ‘anhu) ndipo adadzisungira yekha …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu