20. Musatemberere ana anu pamene mukupempha pa Swalah kapena nthawi ina iliyonse. Ndizotheka kuti temberero lanu litha kukumana ndi nthawi yomwe ma dua amayankhidwa. Olemekezeka Jaabir (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Musadzitemberere nokha, ana anu, akapolo anu, kapena chuma chanu.Temberero lanu likhoza kukumana ndi nthawi (yoyankhidwa) …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 7
18. Popempha mpempheni Mulungu kuti akudalitseni ndi aafiyah (ie kuti akudalitseni momasuka m’magawo onse a moyo wanu). Abbaas (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti: “Nthawi ina ndinamufunsa Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam): “E, Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) wa Allah, ndiphunzitse duwa (yaphindu) imene ndiyenera kupempha kwa Allah. Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) anayankha, “Pemphani …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 6
16.Lekani kulongosora mwatsatanetsatane pa dua yanu. M’malo mwake, muyenera kupempha zabwino zonse. Nthawi ina Abdullah bin Mughaffal Radhwiyallahu anhu anamva mwana wake akupempha m’mawu otsatirawa: “O Allah! Ndikukupemphani nyumba yachifumu yoyera kumbali yakumanja kwa Jannah ndikalowa m’menemo.” Atamva izi Abdullah bin Mughaffal (Radhwiyallahu anhu) adati: “E, mwana wanga! Mpemphe Allah …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 5
12. Mukamaliza dua yanu, nenani Aameen. Abu Musabbih Al-Maqraaiy akusimba kuti: Nthawi ina tidakhala pansi ndi Abu Zuhair An-Numairi (Radhwiyallahu anhu) yemwe anali ochokera mwa ma Swahaabah (Radhwiyallahu anhu). Anali odziwa kulankhula. Aliyense mwa ife akamapempha ankati: “Tsindika duayo ndi mawu oti Aamiin, pakuti Amiin ili ngati chidindo papepala. Kenako …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 4
9. Pamene mukupanga dua, mtima wanu uyenera kukhala olunjika ndi kukhala ndi chidwi kwa Allah, Mtima wanu usakhale osalabadira komanso osaganizira pamene mukupanga dua. Musamamwaze maso kuwayang’ana anthu pamene mukupanga dua. Olemekezeka Abu Hurairah (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Pemphani kwa Allah motsimikiza ndi mwachiyembekezo kuti …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 3
6. Popanga dua, musagwiritse ntchito njira yokayikira. Mwachitsanzo, musanene kuti: “E Allah, ngati Mukufuna kundikwaniritsira zosowa zanga kwaniritsani; Olemekezeka Abu Hurayrah (Radhwiyallahu anhu) adasimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam adati; popanga dua m’modzi wa inu asanene kuti Ndichitireni chifundo ngati Mukufuna, ndikhululukireni ngati Mukufuna ndi ndipatseni mariziki ngati mujufuna.’ m’malo …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 2
2. Popanga dua, kwezani manja anu mofanana ndi pachifuwa chanu (i.e. molingana ndi chifuwa chanu). Olemekezeka Salmaan Faarsi (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: Ndithu Allah ndi olemekezeka, okoma mtima kwambiri komanso owolowa manja. Ulemu Wake ndiwakuti amaona kuti ndi zotsutsana ndi ukulu Wake ndi chifundo Chake …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 1
1. Yambani dua pomulemekeza Allah kenako mudzamuwerengera duruud Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam). Pambuyo pake, modzichepetsa ndi ulemu onse, mudzapempha zosowa zanu pamaso pa Allah. Olemekezeka Fadhaalah bin Ubaid (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti nthawi ina Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) adakhala munzikiti pamene munthu wina adalowa ndikuyamba kuswali. Kenako adapempha nati: “Oh, …
Read More »Nthawi Zomwe Ma Dua Amayankhidwa
Nthawi ya Azaan ndi Pamene Magulu Awiri Akumana Pankhondo Olemekezeka Sahl bin Sa’d (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallah alaihi wasallam) adati: “Pali nthawi ziwiri zomwe madua sangakanidwe kapena nthawi zambiri sangapande osayankhidwa; pa nthawi ya Azaan ndi pamene magulu awiri ankhondo akumana pankhondo.”[1] Pakati pa Azaan ndi Iqaamah Olemekezeka …
Read More »Anthu Omwe Ma Duwa Awo Amayankhidwa 2
Munthu Yemwe Akudwala Olemekezeka Umar (Radhwiyallahu anahu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Mukakumana ndi odwala, mupempheni kuti akupangireni duwa chifukwa dua yake ili ngati dua ya angero (chifukwa cha kudwalako, machimo ake amakhululukidwa), choncho akufanana ndi angelo pokhala opanda machimo, ndipo potero pempho lake lidzalandiridwa mwachangu). Yemwe Amapanga …
Read More »