Daily Archives: July 28, 2025

Kulemekezeka kwa Sa’iid bin Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu) pamaso pa Abdullah bin Umar (radhwiyallahu ‘anhuma)

Tsiku lina Abdullah bin Umar (Radhwiyallahu ‘anhuma) akukonzekera kupita ku Swalaah, adamva kuti amalume ake, Sa’iid bin Zaid (radhiyallahu ‘anhu) akudwala kwambiri ndipo atha kumwalira. Nkhaniyi idamufika pa nthawi yomwe adali atadzola kale (mafuta onunkhiritsa) thupi lake ndipo ali pafupi kuchoka kwawo kupita ku Swalaah ya Jumuah. Koma atamva nkhani …

Read More »