Daily Archives: July 26, 2025

Kuonongeka kwa Ummah asadafike Dajjaal

Zatchuridwa mMahadith kuti Qiyaamah isanafike, khumbo lalikulu la anthu lidzakhala kudzikundikira ndi kusonkhanitsa chuma. Anthu adzachitenga chuma ngati mfungulo ya zinthu zonse zapamwamba ndi chitonthozo, khomo la zosangalatsa zamtundu uliwonse ndi zansangulutso, ndi chida chokwaniritsira zokondweretsa za thupi ndi zilakolako za dziko. Kotero, adzapereka chilichonse kuti apeze ndipo adzachita chilichonse …

Read More »