Salaam ndi moni wa Chisilamu. Monga momwe Chisilamu chimatanthauza mtendere, moni wa Chisilamu ndi moni wamtendere komanso ofalitsa uthenga wamtendere. Salaam ndi imodzi mwa zochitika zachisilamu zomwe ndi chizindikiro cha Msilamu, ndipo kufunika kwake kwatsindikitsidwa kwambiri mahadith. Olemekezeka Abdullah bin Salaam (Radhwiyallahuanhu) akuti: Mtumiki (madalitso ndi mtendere zikhale pa iye) …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu