Nthawi ina pamene ankalankhula za Hazrat Bilaal (Radhiyallahu ‘anhu), Hazrat Sa’eed bun Musayyib (rahimahullah) adati: khumbo lofuna kulowa Chisilamu linali lalikulu kwambiri mu mtima mwa Hazrat Bilaal (radhwiyallahu ‘anhu). Adakumana ndi mavuto ndi mazunzo osalekeza kuchokera kwa anthu osakhulupirira. Nthawi zonse anthu osakhulupirira akafuna kumukakamiza kusiya Chisilamu, iye adali kukana …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu