Daily Archives: September 28, 2025

Tafseer Ya Surah Naazi’aat

وَالنَّازِعَاتِ غَرْقًا ‎﴿١﴾‏ وَالنَّاشِطَاتِ نَشْطًا ‎﴿٢﴾‏ وَالسَّابِحَاتِ سَبْحًا ‎﴿٣﴾‏ فَالسَّابِقَاتِ سَبْقًا ‎﴿٤﴾‏ فَالْمُدَبِّرَاتِ أَمْرًا ‎﴿٥﴾ Ndikulumbirira (angelo) amene amachotsa (mizimu ya osakhulupirira) mwaukali, ndi (angelo) amene amachotsa (miyoyo ya okhulupirira) moleza, ndi (Angelo) amene amasambira nayo mizimuyo (m’mlengalenga), ndi (Angelo) amene amapikisana (kukwaniritsa malamulo a Allah Ta’ala). Monga ziliri kuti Sura Nabai idavumbulutsidwa kuti idzakhazikitse chikhulupiriro cha tsiku la …

Read More »