27. Wina asapereke salaamu pomlonjera munthu amene si Msilamu. Ngati amene sali Msilamu apereka moni wa salaamu, ayankhe pongonena kuti “Wa alaik” (ndi pa inu), ndipo ngati ambiri omwe si Asilamu apereka salaam kwa munthu, ayenera kuyankha kuti “Wa alaikum” (ndi kwa inu nonse). 28. Akakumana Asilamu awiri, akamaliza salaam, …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu