Daily Archives: September 25, 2025

Sunnats Ndi Aadaab Za Salaam 10

30. Popanga musaafah, ingogwirani manja a munthuyo, Palibe chifukwa chogwirana chanza ndikumavinitsa monga amachitira ma kuffaar. Chimodzimodzinso sizoyenera kupanga musaafahah uku ndikumapsopsona dzanja lake ndikumasisita pachifuwa chake popeza machitidwewa alibe maziko mu Dini. 31. Popanga musaafah, musagwire manja a munthu winayo momufinya mpaka kumupweteka. 32. Musafulumire kuchotsa manja anu mukapanga …

Read More »