Tsiku la Jumu’ah ndi lofunikira kwambiri mu Chisilamu. Izi ndi zina mwa zabwino zazikulu za Allah pa Ummah uwu ndipo ndichinthu chodziwika bwino m’Chisilamu. Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) adati: “Tsiku la Jumu’ah ndi sayyidul ayyaam (lomwe ndi mtsogoleri wa masiku onse), ndi tsiku lalikulu kwambiri (kuchokera m’masiku a msabata) pamaso …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu