Jumuah

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 4

11. Werengani durood mochuluka. Olemekezeka Aws bin Aws radhwiyallahu anhu akufotokoza kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Masiku abwino kwambiri ndi tsiku la Jumuah. 12. Yesetsani kuwerenga duruud chikwi chimodzi (ka 1000) tsiku la Jumuah. Olemekezeka Anas radhwiyallahu anhu akusimba kuti Mtumiki swallallahu alaihi wasallam adati: “Amene amawerenga duruud pa …

Read More »

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 3

9. Ngati n’kotheka, yendani wapansi popita ku musjid kukaswali swalaah ya Jumu’ah. Phanzi lirilonse lomwe mungaponye, mudzalandira mphotho ya kusala kudya kwa chaka chimodzi ndi Tahajjud. Olemekezeka Aws bin Aws Thaqafi radhwiya-Allah anhu akuti, “Ndidamva Rasulullah swallallahu alaihi wasallam akunena kuti, ‘Munthu amene amachita ghusl tsiku la Jumu’ah ndipo amapita …

Read More »

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 2

8. Pitani mwamsanga ku mzikiti kukaswali Jumu’ah, momwe mungapitire mwamsanga ndi momweso mungalandilire mphotho yochuluka. Olemekezeka Abu Hurairah radhwiya-Allahu ‘anhu akusimba kuti Rasulullah swallallahu alaihi wasallam adati, “Amene amasamba ngati momwe amasambira akakhala ndi janaabah (i.e. amasamba mosamaritsa monga momwe amachitira akakhala ndi janaabah), ndikupita ku Jumu’ah Salaah moyambilira, amalandira …

Read More »

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 1

1. Werengani Surah Dukhaan Lachinayi usiku. Olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallah anhu) akunena kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati, munthu amene amawerenga Surah Haa-meem Ad-Dukhaan usiku wa Jumu’ah ( Lachinayi usiku), machimo ake adzakhululukidwa.” 2. Sambani (ghusl) Lachisanu. Munthu amene amasamba Lachisanu, machimo ake ang’onoang’ono amakhululukidwa. Olemekezeka Abu Bakr Siddeeg (radhwiyallahj …

Read More »

Ubwino wa Jumuah

Kukhululukidwa Kwa Machimo kudzera mukuswali Jumuah Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Machimo omwe achitika pakati pa Jumu’ah ziwiri, ngati sali machimo akuluakulu, Allah amakhululuka. Tsiku Lopatulika kwa Okhulupirira Ibnu Abbaas (radhwiyallahu anhuma) adanena kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Tsiku ili (tsiku la Jumu’ah) …

Read More »

Jumuah

Tsiku la Jumu’ah ndi lofunikira kwambiri mu Chisilamu. Izi ndi zina mwa zabwino zazikulu za Allah pa Ummah uwu ndipo ndichinthu chodziwika bwino m’Chisilamu. Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) adati: “Tsiku la Jumu’ah ndi sayyidul ayyaam (lomwe ndi mtsogoleri wa masiku onse), ndi tsiku lalikulu kwambiri (kuchokera m’masiku a msabata) pamaso …

Read More »