Daily Archives: January 24, 2026

Momwe Adabadwira Nabi Isa (‘alaihis salaam)

Dongosolo la Allah Ta‘ala, kukamba momwe amalengedwera anthu, ndilakuti anthu awiri akakumana munthu amapangidwa. Chinthu choyamba ndi kudzera mwa makolo omwe mbewu ya mwamuna imabzalidwa m’mimba mwa mayi. Chinthu chachiwiri ndi mzimu omwe umalowa m’mimba mwa mwana yemwe sanabadweyo akakwanitsa miyezi inayi. Munthu aliyense amene anabwera padziko lapansi adatsatira njira …

Read More »