Monthly Archives: December 2025

Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Jumu’ah 4

11. Werengani durood mochuluka. Olemekezeka Aws bin Aws radhwiyallahu anhu akufotokoza kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Masiku abwino kwambiri ndi tsiku la Jumuah. 12. Yesetsani kuwerenga duruud chikwi chimodzi (ka 1000) tsiku la Jumuah. Olemekezeka Anas radhwiyallahu anhu akusimba kuti Mtumiki swallallahu alaihi wasallam adati: “Amene amawerenga duruud pa …

Read More »

Kusalilabadira kwa Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu) Ddziko Lapansi

Abu Zar Ghifaari (Radhwiyallahu ‘anhu) anali Sahaabi yemwe ankafanana ndi Nabiy Isa (‘alaihis salaam) m’maonekedwe ake komanso kukongola kwake. Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) anati, “Aliyense amene akufuna kumuona Isa bin Maryam (‘alaihis salaam) Taqwa yake, chilungamo chake, ndi kudzipereka kwake (pa ibaadah), ayenera kumuyang’ana Abu Zar” (Majmauz Zawaaid #15817) Chimodzimodzinso, …

Read More »