Mahdi atabwera, Allah Ta‘ala adzawapatsa Asilamu uysogoleri ndi mphamvu padziko lonse lapansi. Akristu adzazindikira kuti Asilamu akupeza thandizo ndipo akukula mphamvu tsiku ndi tsiku. Kenako adzakonza gulu lankhondo lalikulu kuti amenyane ndi Mahdi ndi Asilamu. Zanenedwa mu Hadith kuti Akristu ochokera m’maiko onse adzasonkhanitsa asilikali awo ndikukonzekera kumenyana ndi Asilamu. …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu