6. Pangani ma dua komanso azkaar musanagone; اللَّهُمَّ بِاسْمِكَ أَمُوْتُ وَأَحْيٰ O, Allah Talaa mdzina Lanu ndikufa komanso ndiuka 7. Gonerani kumanja ndikuika dzanja lanu lamanja pansi pa tsaya lanu lakumanja. Bibi Hafsah (radiyallahu anha) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) akafuna kugona, ankaika dzanja lake lamanja pansi pa tsaya …
Read More »Monthly Archives: June 2026
Munthu Olungama Kwambiri – Fudhail Bin Iyaaz Rahimahullah
Fudhail bun Iyaaz (Rahimahullah) aDali Muhaddith olemekezeka komanso oyera mtima wa m’nthawi yake. Allah Talaa adamdalitsa ndi ulemelero wapamwamba kwambiri mu Hadith kotero kuti ambiri mwa ma Muhadith otsogola, monga Abdullah bin Mubaarak, Sufyaan bun Uyainah ndi Imaam Shaafi’e (Rahimahullah) adafotokoza Hadith kuchokera kwa iye. Zanenedwa kuti Fudhail (Rahimahullah) asanadalitsidwe …
Read More »Rasulullah (Swallallahu ‘alaihi wasallam) Amuitana Abdullah bin Mas’ud (radhwiyallahu ‘anhu) ku Moyo Osatha
Salamah bin Tammaam (rahimahullah) akufotokoza kuti: Masiku angapo Abdullah bin Mas’ud (radhiyallahu ‘anhu) asanamwalire, munthu wina adabwera kudzakumana naye. Atakumana naye, munthuyo anamuuza kuti, “Oh Ibnu Mas’ud! Usiku watha, ndinakulota. M’maloto, ndinamuona Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) atakhala pa guwa pomwe iwe unali pansi pake. “Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) anakulankhula nanu …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu