Daily Archives: June 9, 2026

Munthu Olungama Kwambiri – Fudhail Bin Iyaaz Rahimahullah

Fudhail bun Iyaaz (Rahimahullah) aDali Muhaddith olemekezeka komanso oyera mtima wa m’nthawi yake. Allah Talaa adamdalitsa ndi ulemelero wapamwamba kwambiri mu Hadith kotero kuti ambiri mwa ma Muhadith otsogola, monga Abdullah bin Mubaarak, Sufyaan bun Uyainah ndi Imaam Shaafi’e (Rahimahullah) adafotokoza Hadith kuchokera kwa iye. Zanenedwa kuti Fudhail (Rahimahullah) asanadalitsidwe …

Read More »