Olemekezeka Umar (Radhwiyallaahu ‘anhu) adanenapo nthawi ina kwa olemekezeka Abbaas (Radhwiyallahu ‘anhu) (amalume a Rasulullah (Swallallaahu ‘alayhi wasallam)) kuti: “Ndidakondwera ndi Chisilamu chanu kuposa Chisilamu cha abambo anga chifukwa Chisilamu chanu chidabweretsa chisangalaro chochuluka kwa Rasulullah swallallahu ‘alaihi wasallam) kuposa Chisilamu cha bambo anga. (Sharhu Ma’aanil Aathaar 3/321)
Audio PlayerCheck Also
Kuwolowa manja kwa Abdur Rahmaan bin Auf (Radhiyallahu ‘anhu)
Miswar bin Makhramah (Radhwiyallahuanhu) akuti: Abdur Rahmaan bun Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) nthawi ina adagulitsa munda …