Chisangalalo cha Hazrat Umar (Radhiyallahu ‘anhu)

Olemekezeka Umar (Radhwiyallaahu ‘anhu) adanenapo nthawi ina kwa olemekezeka Abbaas (Radhwiyallahu ‘anhu) (amalume a Rasulullah (Swallallaahu ‘alayhi wasallam)) kuti: “Ndidakondwera ndi Chisilamu chanu kuposa Chisilamu cha abambo anga chifukwa Chisilamu chanu chidabweretsa chisangalaro chochuluka kwa Rasulullah swallallahu ‘alaihi wasallam) kuposa Chisilamu cha bambo anga. (Sharhu Ma’aanil Aathaar 3/321)

Check Also

Abu Zar (radhiyallahu ‘anhu) Apereka Uphungu kwa Mtsogoleri wa Asilikali Kuti Atsatire Chilungamo

Imaam Bayhaqi (rahimahullah) akunena kuti: Yazid bin Abi Sufyaan (radhiyallahu ‘anhu) pamene adali bwanamkubwa wa …