Olemekezeka Talhah (Radhwiyallaahu ‘anhu) akuti: Ma Swahaabah (Radhwiya Allahu ‘anhum) adauza munthu wina okhala kumudzi kuti: “Pita ukafunse kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) kuti Allah Ta’ala akunena za ndani (m’ndime yotsatira ya Quraan Majeed)” (ma Sahaabah) ndi amene adakwaniritsa lonjezo lawo (ndi Allah Ta’ala lokhala okhazikika pankhondo okonzeka kupereka …
Read More »Olemekezeka Talhah (Radhiyallahu ‘anhu) pa Nkhondo ya Uhud
Olemekezeka Jaabir bin Abdillah (Radhwiya Allaahu ‘anhu) adati: Pa tsiku la nkhkndo ya Uhud, pamene ma Swahaabah adayamba kuthawa kunkhondo, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adasiidwa yekha pamalo ena ndi ma Swahaaba khumi ndi awiri okha.) Ma mushrikiin atapita kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) ndi ma Swahaabah khumi ndi …
Read More »Chisilamu cha Olemekezeka Talhah bin Ubaidillah (Radhwiyallahu ‘anhu)
Tsiku lomwe sayyiduna Abu Bakr Siddeeq (Radhwiyallahu ‘anhu) adalowa Chisilamu, adayamba kuyitanira anthu ku Chisilamu, Allah Ta’ala adamupanga kukhala njira ya ma Swahaabah (radhwiyallahu ‘anhun) ambiri kulowa Chisilamu. Mwa ma Swahaabah amene adalowa Chisilamu kudzera mwa Abu Bakr Siddeeq (radhwiyallahu ‘anhu) anali Talhah bin Ubaidillah (radhwiyallahu ‘anhu). Talhah (radhwiyallahu ‘anhu) …
Read More »Kuolowa Manja kwa Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu)
Ali bin Zayd (Rahimahullah) akusimba kuti nthawi ina yake, Nchikumbe wina adapita kwa Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) kuti akapemphe thandizo kwa iye. Nchikumbeyu kudapezeka zoti adali m’bale wake wa Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) ndipo popereka pempho lake, adamupempha kudzera mu ubale omwe udalipo pakati pawo. Talha (Radhwiya Allaahu ‘anhu) adayankha: “Kupatula Inu, …
Read More »Mantha a Olemekezeka Talha (radhwiyallahu annhu) kuopa kuti Chuma cha Padziko Lapansi chisamuchititse Osakumbukira Allah Ta’ala.
Nthawi ina, Olemekezeka Talha (radhwiyallahu anhu) adalandira ndalama zokwana ma dirham zikwi mazana asanu ndi awiri kuchokera ku Hadhramaut. Kutada usiku, atagona, iye anasowa mtendere, kumangotembenuka kuchoka mbali Ina kupita uku. Poona kukhumudwa kwake, mkazi wake adamufunsa, “Nchiyani chikukuvutitsani, iye adayankha “Kodi munthu angaganize bwanji za Rabb pomwe ali ndi …
Read More »Olemekezeka Talhah pa Nkhondo ya Uhud
Sayyiduna Zubair bun Awwaam Radhwiyallahu anhu ananena kuti pa nkhondo ya Uhud, Rasulullah swallallahu alaih wasallam adavala zovala zodzitetezera ziwiri mophatikiza. Pankhondoyi, Rasulullah ankafuna kukwera pa thanthwe koma chifukwa cha kulemera kwa zovalazo adalephera kutero. Choncho adamupempha Talhah Radhwiyallahu anhu kuti akhale pansi kuti amuthandizire kuti akwere pa thanthwepo. Talhah …
Read More »Ulemelero Wapamwamba wa Abu Ubaidah (Radhwiyallahu ‘anhu) Pamaso pa Abu Bakr (Radhwiyallahu ‘anhu)
Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) atamwalira, ma Ansaar adasonkhana ku Saqeefah Bitti Saa’idah m’munda wa zipatso wa Bani Saaidah) kuti asankhe khaleefa pakati pawo. Nthawi imeneyo Abu Bakr ndi Umar anali m’nyumba ya Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) ndipo sankadziwa zomwe zinkachitika. Ali m’nyumbamo, Umar mwadzidzidzi adamva mawu kuitana …
Read More »Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) Awonetsa ku Ummah Udindo olemekezeka wa Abu Ubaidah (radhiyallahu ‘anhu)
Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) Awonetsa ku Ummah Udindo olemekezeka wa Abu Ubaidah (radhiyallahu ‘anhu) Ranılullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adakhala pamodzi ndi Abu Bakar (Radhwiyallahu ‘anhu), Umar (Radhwiyallahu ‘anhu), Abu Ubaidah (Radhwiyallahu ‘anhu) ndi maSwahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum). anapatsidwa chakumwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi …
Read More »Kuopa Allah Taala
Qataadah (Rahimahullah) akusimba kuti Olemekezeka Abu Ubaidah (Radhwiyallahu ‘anhu) ankati, (chifukwa choopa kudzaima pamaso pa Allah Ta’ala pa tsiku la Qiyamah ndi kuwerengetsedwa ntchito zake. وددت أني كنت كبشا، فيذبحني أهلي، فيأكلون لحمي، ويحسون مرقي. “Ndikulakalaka ndikadakhala nkhosa. Ondipha akadandipha, akanadya nyama yanga ndikumwa nsuzi wanga. (Siyaru Aa’laamin Nubalaa 3/14) …
Read More »Kudzipatula kwa Olemekezeka Abu Ubaidah (Radhwiyallahu ‘anhu) ku Chuma Chadziko Lapansi
Umar (Radhiyallahu ‘anhu) atachoka ku Madina Munawwarah kupita ku Baitul Muqaddas kuti akagonjetse, adayima ku Syria kuti akakumane ndi ma Swahaabah omwe ankakhala kumeneko. MaSwahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) adadzakumana naye (Radhwiya Allahu ‘anhu) yemwe adali kukhala ku Syria ndi kulamulira Syria, adawafunsa: “Ali kuti m’bale wanga?” maSwahaabah (Radhwiyallahu ‘anhu) adafunsa: “Kodi …
Read More »