Abu Muslim Khowlaani (rahimahullah) akufotokoza kuti: “Ndinalowa mumzikiti wa Hims ndipo ndinaona gulu la anthu. Pakati pawo panali anzake makumi atatu ndi awiri a Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) omwe ankakambirana za mahadith kuchokera kwa Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam). Munkumanowu munali mnyamata, amene maso ake anali atapakidwa surma ndipo mano ake …
Read More »Chikondi cha Rasulullah (Sallallahu ‘alaihi wasallam) kwa Sayyiduna Muaaz bin Jabal (radhiwyallahu ‘anhu)
Sayyiduna Muaaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) akunena kuti nthawi ina, Nabi (Swallallahu alaihi wasallam) anagwira dzanja langa nati kwa ine, “O Muaaz!”, ndipo ine ndinayankha kuti, “Ndili pano kuti ndikutumikireni.” Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) kenako anandiuza kuti, “Ndithudi, ndimakukonda (chifukwa cha Allah Ta’ala).” Muaaz bin Jabal (Radhwiyallahu ‘anhu) anayankha kuti, …
Read More »Muaaz (radhwiyallahu ‘anhu) Aswa fano la Amr bin Jamuuh (radhwiyallahu ‘anhu)
M’chaka cha 13 cha nubuwwat, anthu 70 ochokera ku Ansaar anabwera ku Hajj ndipo analowa Chisilamu pamaso pa Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam). Pakati pawo panali Muaaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) yemwe anali ochokera ku fuko la Banu Salimah la Ansaar, ndipo anali m’gulu la anthu oyambilira ku fuko lawo kulowa …
Read More »Kupereka kwa Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu)
Nthawi ina,Olemekezeka Umar (radhwiyallahu ‘anhu) anatumiza ndalama zagolide mazana anayi kwa Abu ‘Ubaidah bin Jarraah (radhwiyallahu ‘anhu) ndipo analamula mthumwiyi kuti ikadikire pang’ono kuti aone zomwe achite nacho chumacho. Olemekezeka Abu Ubaydah (radhwiyallahu ‘anhu) atalandira ndalamazo, anati, “Allah amuchitire chifundo (kunena Umar).” Kenako anauza kapolo wake wamkazi kuti, “Tenga ndalama …
Read More »Rasulullah (Swallallahu ‘alaihi wasallam) Amuitana Abdullah bin Mas’ud (radhwiyallahu ‘anhu) ku Moyo Osatha
Salamah bin Tammaam (rahimahullah) akufotokoza kuti: Masiku angapo Abdullah bin Mas’ud (radhiyallahu ‘anhu) asanamwalire, munthu wina adabwera kudzakumana naye. Atakumana naye, munthuyo anamuuza kuti, “Oh Ibnu Mas’ud! Usiku watha, ndinakulota. M’maloto, ndinamuona Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) atakhala pa guwa pomwe iwe unali pansi pake. “Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) anakulankhula nanu …
Read More »Kusamalitsa kwakukulu Kwa Sayyiduna Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) Potulutsa mahadith a Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam)
Ole.wkezeka ‘Amr bin Maimoon (rahimahullah) adafotokoza za kusamalitsa kwakukulu kwa Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) pamene ankatulutsa mahaadith kuchokera kwa Rasulullah (ssallallahu alaihi wasallam). Adanena kuti, “Nthawi ina, Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) atayamba kunena Hadith yochokera kwa Rasulullah (sallallahu alaihi wasallam), adagwidwa ndi mantha ndi nkhawa kotero kuti madontho …
Read More »Hazrat Abdullah bin Mas’uud (radhiyallahu ‘anhu) ndi Izindikiri wake a Quraan Majiid
Shaqiiq bin Salamah (rahimahullah), ophunzira wa Abdullah bin Mas’uud (radhiyallahu ‘anhu), akunena kuti nthawi ina yake, Abdullah bin Mas’uud (radhiyallahu ‘anhu) adapereka khutbah. Mu khutbahmo adati, “Ndikulumbira qasam mwa Allah! Ndinaphinzira ma surah oposa makumi asanu ndi awiri a Quraan Kariim mwachindunji kuchokera kwa Rasulullah (sallallahu alaihi wasallam). Ndikulumbira m’dzina …
Read More »Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) amupempha Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) kuti amuwerengere Quraan Majeed
Nthawi ina, Rasullullah (Swallallahu alaihi wasallam) anabwera ku fuko la Bani Zafar (fuko lachi Ansaar). Ali pa mimbar akulankhula nawo, anamuuza Abdullah bin Mas’ood (radhwiyallahu ‘anhu), kuti, “Ndiwerengere Quraan.” Modzichepetsa kwambiri, Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) anauza Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam), “Eh Mtumiki wa Allah, kodi ndikuwerengereni kumachita kuti Quraan …
Read More »Chitsimikizo Cha Sayyiduna Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) Pa Mawu a Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam)
Ulendo wina, nthawi ya khilaafat yake, Sayyiduna Uthmaan (radhwiyallhu ‘anhu) anabwera kudzacheza ndi Olemekezeka Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu). Apa ndikuti Abdullah bin Masood (radhwiyallahu ‘anhu) akudwala matenda ake omaliza. Sayyiduna Uthman (radhwiyallahu ‘anhu) anamufunsa kuti, “Ndi vuto lanji lomwe likukusautsa?” Abdullah bin Mas’ood (radhiyallahu ‘anhu) anayankha kuti, “Chomwe chikundisautsa …
Read More »Hazrat Abdullah ibn Mas’uud (radhiyallahu anhu) Kuwerenga Qur’aan Majeed mokweza mawu pamaso pa Aquraish
Hazrat Abdullah ibn Mas’uud (radhiyallahu anhu) adali munthu oyamba kuwerenga Qur’aan Majeed mokweza mawu ku Makkah Mukarramah Aquraish asanalowe Chisilamu. Tsiku lina, maSwahaabah (radhiyallahu anhum) anasonkhana nati, “Ndikulumbira mwa Allah, Aquraish sanamvepo wina akuwerenga Qur’aan mokweza mawu pamaso pawo, ndiye ndani pakati pathu amene ali okonzeka kupita kukawerenga Qur’aan mokweza …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu