Nthawi ina Rasulullah (Swalla-Allaahu ‘alayhi wasallam) adamufunsa Busrah bint Safwan (Radhwiya-Allahu ‘anha) kuti ndi ndani amene ankafuna kukwatira mphwake, Umm Kulthuom bint Uqbah. Adamufotokozera mayina a anthu ochepa omwe adamfunsira mphwakeyo, ndipo adamuwuzanso kuti mwa anthu omwe adamfunsira mphwakeyo ndi Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu). Zitatero, Mtumiki (Swalla-Allaahu ‘alayhi …
Read More »Yearly Archives: 2025
Ubwino Osiya Pambuyo Mwana Olungama
Bambo a Nabii Yunus (alayhis salaam) adali munthu Owopa Allah dzina lawo Mattaa. Iwo ndi mkazi wawo kwa nthawi yaitali ankafuna kuti Allah atawadalitsa ndi mwana wamwamuna ndi kumuchita kukhala Mneneri kwa Bani Israeil. Zaka zambiri zidadutsa uku akumapempha mpaka pamapeto pake adaganiza zopita kukasupe odalitsika wa Nabii Ayyoob komwe …
Read More »Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu pa Nkhondo ya Uhud
Pankhani ya kupirira kwa Talha (Radhwiyallahu ‘anhu) pankhondo ya Uhud, Sa’d bin Abi Waqqaas (Radhwiyallahu ‘anhu) adanena izi: Allah Ta’ala amuchitire chifundo Talha. Mosakayikira, mwa ife tonse, adamuthandiza kwambiri Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wa wasallam) pa tsiku la Uhud. Kenako Sa’d (Radhwiyallahu ‘anhu) adafunsidwa: “Tifotokozere momwe (adamuthandizira kwambiri Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi …
Read More »Ubwino Oyendera Odwala 1
Kupeza Mwayi Opangiridwa Dua Ndi Angelo Okwana Zikwi Makumi Asanu Ndi Awiri (70,000) Olemekezeka Ali (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Amene amayendera odwala m’bandakucha, angero zikwi makumi asanu ndi awiri (70,000) amamupemphera chifundo kwa Allah mpaka madzulo; Amene angamuyendere odwala madzulo angelo okwana 70,000 amamupemphera chifundo …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu