Ma’roor bin Suwaid (rahimahullah) akufotokoza izi: Nthawi ina tinadutsa kwa Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu) ku Rabzah ndipo tinaona kuti anali atavala zovala ziwiri. Chimodzi chinali chakale, pomwe china chinali chatsopano, ndipo kapolo wake nayenso anali atavala zovala ziwiri, zomwe chimodzi chinali chatsopano ndipo china chinali chakale. Kenako tidati kwa Abu …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu