Daily Archives: November 25, 2025

Makolo Kutsogolera Mwa Chitsanzo

Rasulullah swallallahu alaihi wasallam anali olemekezeka kwambiri pa zolengedwa za Allah, Allah adamusankha kukhala Mtumiki Wake omaliza ndipo adamudalitsa ndi dini yolemekezeka kwambiri – dini ya Chisilamu yomwe ndi malamulo abwino kwambiri a moyo kuti munthu atsatire. Munthu akalingalira pa umunthu odalitsika wa Rasulullah swallallahu alaihi wasllam amapeza kuti Allah …

Read More »