Daily Archives: November 8, 2025

Momwe Mungadzipulumutsire ku Fitnah (Mayesero)za Dajjaal

M’mahadith odalitsika, Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adaupatsa ummah mankhwala odzitetezera ku ma Fitna a nthawi zonse komanso Mayesero a Dajjaal. Zanenedwa kuti Olemekezeka Uqbah bin Aamir (radhwiyallahu ‘anhu) nthawi ina adamufunsa Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam), “Oh Rasul wa Allah (swallallahu ‘alaihi wasallam)! Kodi njira yopezera chipulumutso ndi iti (kuchokera ku …

Read More »