Zidatengera Abu Zarr Ghifaari (radhiyallahu ‘anhu) kuphunzira moyo wa Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) osasamala za moyo wadziko lapansi komanso kudziletsa ndi kumvera machenjezo amphamvu kwa omwe ali ndi chuma koma osagwiritsa ntchito moyenera, Abu Zarr (radhwiyallahu ‘anhu) adayamba kudana ndi dziko lapansi kotero kuti sanasunge chuma ndipo sankakonda kuona anthu …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu