11. Werengani durood mochuluka. Olemekezeka Aws bin Aws radhwiyallahu anhu akufotokoza kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Masiku abwino kwambiri ndi tsiku la Jumuah. 12. Yesetsani kuwerenga duruud chikwi chimodzi (ka 1000) tsiku la Jumuah. Olemekezeka Anas radhwiyallahu anhu akusimba kuti Mtumiki swallallahu alaihi wasallam adati: “Amene amawerenga duruud pa …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu