Kubwera kwa Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu) ndi chizindikiro choyamba mwa zizindikiro zikuluzikulu zomwe zidzawonekere Qiyaamah isadafike. M’mahadith odalitsika ambiri, Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adalosera za kubwera kwa Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu) ku ummah uno. Allaamah Suyuuti (rahimahullah) wafotokoza kuti mahadith okhudzana ndi kubwera kwa Mahdi (radhwiyallahu ‘anhu) ndi ochuluka kwambiri kotero kuti …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu