Sayyiduna Muaaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) akunena kuti nthawi ina, Nabi (Swallallahu alaihi wasallam) anagwira dzanja langa nati kwa ine, “O Muaaz!”, ndipo ine ndinayankha kuti, “Ndili pano kuti ndikutumikireni.” Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) kenako anandiuza kuti, “Ndithudi, ndimakukonda (chifukwa cha Allah Ta’ala).” Muaaz bin Jabal (Radhwiyallahu ‘anhu) anayankha kuti, …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu