Dajjaal akadzaonekera padziko lapansi, adzayamba kutulukira ndi kum’mawa kwa dziko, pakati pa Syria ndi Iraq. Pambuyo pake, adzapita ku Isfahaan komwe Ayuda 70,000 adzakhale naye limodzi. (Muslim #2944) Adzayenda padziko lonse lapansi, ndipo kulikonse komwe akupita, adzabweretsa fitnah yaikulu komanso ziphuphu zambiri. Malo awiri okha omwe sadzatha kulowamo ndi Makkah …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu