Daily Archives: July 13, 2026

Mtumiki (Swallallahu ‘alaihi wasallam) asankha Mu’aaz bin Jabal (radhwiyallahu ‘anhu) kukhala Bwanamkubwa wa Yemen

Rasulullah (Swallallahu ‘alaihi wasallam) pomutumiza Mu’aaz (radhwiyallahu ‘anhu) ku Yemen, adamufunsa kuti, “Ndi njira yanji yomwe udzatsatire ukamakapereka chigamulo pa nkhani za Asilamu?” Mu’aaz (Radhwiyallahu ‘anhu) adayankha kuti: “Ndidzagwiritsa ntchito Qur’aan.” Kenako Nabi (Swallallahu ‘alaihi wasallam) adamufunsa kuti: “Ngati lamulo silikupezeka mu Qur’aan udzatani?” Iye adayankha kuti, “Ndidzagwiritsa nctchito mahaadith …

Read More »