7. Osamwera mbali yomwe ndi yodulidwa kapena yosweka ya chikho, chifukwa ndizotheka kuti mutha kuvulala. Olemekezeka Abu Sa’eed Khudri (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adamuletsa munthu wina kumwera mbali ya chikho yophwanyika kapena kusweka. 8. Musauzire m’pweya m’chiwiya. Sayyiduna Ibnu Abbaas (radhwiyallahu anhuma) akunena kuti Rasulullah (swallallahu …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu